Email a copy of 'Malawi First Lady no show as Joyce Banda address conference in New York' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

129 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
KKKKKK
KKKKKK
9 years ago

Koma kunena chilungamo apapa yakula ndi nsanje. They know JB is not their match internationally. If you JB haters do not accept kuti JB sinzanu, zanu izo. Think of the past first ladies and their trusts which ends when the presidency of their spouses come to an end because of lack of vision on how to make them survive. And think of NABW, JB Foundation and now JBFAI which has just been launched. What does all this tells you about the woman behind these foundations?. What does the unending international invitations to different forums tells you? If I were the… Read more »

Weekly mwale
9 years ago

The first lady must really appreciate the good work being done by jb.its an honour for malawi to have its former president chairing such a gathering.being a malawian the first lady must feel proud of jb instead of a boycott. When malawians went to the elections they spoke through the ballot.pliz those who lost stop throwing spanners. Wait for your chance to come. Stop hatred you malawians have never tasted blood shed. Stop this nosense! Before you burn this beautiful country into ashes.~weekly mwale is a zimbabwean whose parents originated from nkhata bay.

Mwana ovuta
9 years ago

Iwe getu, ukungonyanyala zopandapake. Anzanu anzeru akuganiza zotukula malawi n africa iwe ungoganiza zonyanyala meetings zithandizapoapa kaya a DPP MUYISOVA NOKHA.

yohane munthali
yohane munthali
9 years ago

KOMA ZINAZI JB TAMAKHALANI NDI MANYAZI PENAPAKE, MPAKA LONDOLONDO…MWINA NTHAWI ZINAKUKANIKANI KUTI MUKATHILE UJENI KU STATE HOUSE PONAMIZIRA KUTI MUNAYIWALA KATUNDU WANU KU STATE HOUSE…NDE MWATI MUMSATIRE PETER KU USA KOMWEKO MUKAMPANGE UJENI….TIKUKUWERENGANITU.BECAREFUL

Tayani
Tayani
9 years ago

hmmmmmmmmmmmmmmmmmmm .anthu inu taziyamikani .nsanjeyi ndi imene amalawi tikutsalira nayo. nsanje nsaje eeeeeeeeeeeeeeeeeeeee

yohane munthali
yohane munthali
9 years ago

KOMA ANTHU INU,MUTISANDIPWETEKETSE IFE MA LECTURE OMWE TILI ATUMBUKA MU MA UNIVERSITY KUNO KU SOUTH CHFUKWA CHA FIDERAL GOVERNMENT,BOMA LA CHITAGANYA MUKANGOVOMEREZA IFE ATUMBUKA TONSE OMWE TIKUGWIRA NTCHITO KU SOUTH NDI CENTRAL REGION TIZATHAMANGISIDWA KUBWELERA KWATHU KU NORTH…KOMANSO ANA ATHU OMWE ALI MA UNIVERSITY KU SOUTH NDI CENTRAL AZAWATHAMANGITSANSO…NDE MUGANIZE BWINO NDI KACHIGAWO KATHU KA NORTH NDIKAKAN’GONO KWAMBIRI…PLIZZZZZZZ…..MUSATIPALAMULIRE MOTO KAMUZU ANATHETSA KALE CHITAGANYACHO……KODI LAZARO CHAKWERA KODI UKUFUNA UTIPWETEKETSE NDI CHITAGANYA?BOLANSO JOHN TEMBO YEMWE UJATU….TSOKA KWA IYE WOYAMBITSA MAVUTO…MASIKU OTSILIZA AMWENEWA…MMMMMM?BOLA JOHN TEMBO AZIBUSA AYAMBA KUOPSADI…MPAKA CHAKWERA NDI NGWIRA KUBWELETSA ZIWAWA CHIFUKWA CHA CHITAGANYA…VOTI YANGA IZAKUTIPULA PA 2019 ELECTION…INE NTCHITO NDANGOYAMBA… Read more »

Tayani
Tayani
9 years ago

mabodza amenewo iwe .you are not a tumbuka.

anambewe
anambewe
9 years ago

Madam Getrude dont be selfish you need to appreciate what JB is doing and achieving, if you want things to go well learn from others. The Holy spirit must guide you, Amen.

James perenje
9 years ago

Kkkkkkkkkk anthu kunyoza basi mumatha

Kwizman
Kwizman
9 years ago

JB fire!!!

VYOTO
VYOTO
9 years ago

INDEED THE WORKS OF ONE OF THE MOST POWERFUL WOMEN IN AFRICA! IF TRUTH BE TOLD DURING JOYCE BANDA’S FIRST 5 MONTHS AS PRESIDENT SHE DID QUITE A LOT TO THE BENEFIT OF MANY MALAWIANS INCLUDING PETER MUTHALIKA.DONORS THAT HAD DESERTED MALAWI BECAUSE OF POOR GOVERNANCE OF LATE BINGU WERE BROUGHT BACK AND IN THE PROCESS FOREX PROBLEMS BECAME A THING OF THE PAST.FUEL PROBLEMS WERE RESOLVED BY BRINGING IN AUTOMATIC FUEL PRICING SYSTEM WHICH PETER MUTHALIKA IS ALSO USING UP NOW YET HIS LATE BROTHER BINGU AND DPP ARROGANTLY REJECTED IT.JB ALSO HAD TO UNDERSTAND AND AGREE WITH THE… Read more »

bambala
bambala
9 years ago

Za Chamba basi, or atanyanyala ife zitithandizapo chani First lady wanuyo. Bweraniko kuno muzakumane ndi ma civil servant akufuna increament kuno, Passport k40,000.00. federalism debate ikumudikilanso kuno or muchoneko kumeneko, a Malawi muzawapezabe basi.

Read previous post:
It’s Silver, Epac final in Be Forward tourney: Bullets, Nomads fall

A 78th minute own goal  conceded by Jafali Chande was enough to send his team Big Bullets football club out...

Close