Email a copy of 'Malawi Gaming Board warns of unlicensed betting like ‘Wachionandani’' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Malawi Gaming Board warns of unlicensed betting like ‘Wachionandani’' to a friend
Mphatso Nkhoma -Nyasa Times Leader of opposition People’s Party (PP) in parliament and its acting president Uladi Mussa has blasted...
Azimayi ambiri ndi amene akudyetsa ndalama za ngati zimenezi.
Juga ya wachionandani imayamba nthawi ino, mwaiganiza.
Juga yolipira imathandiza dziko, mchifukwa chake muone ngakhale kunja MANU, Chelsa ndi Livermbuzi amapanga juga ndipo zimathandiza ma team awo. Inu a Wanderers yambanipo kuti muzithandiza kalabuyo.
Kodi juga ndi yoloredwa Mmalawi muno? Nanga woyenera kulowa ndani? Ambiri akutayitsa ndalama zao pachabe.
This game must be discarriaged as most women loose their monies, bravo MGB