Email a copy of 'Malawi gospel singer King James Phiri sued – Zodaik reports' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Malawi gospel singer King James Phiri sued – Zodaik reports' to a friend
Chewa Heritage honoree and rapper Tay Grin had his Independence Day performance at Kamuzu Stadium put off-air on Monday. The...
mwazolowera zimenezi ..ku show anthu kulowa mwaunyinji ar tist yo osabwera. This is a lesson
Musamuonongere cv mzanu inu a odala. Mukakambirana zinthu zimayenda bwino osati kuopseza ndi court. Next time ena adzakukanani. Mukopa bwanji omwe sanamulandire Yesu, ndi khalidwe mwachitali?osadandaula kwa akuluakulu a gulu la ma gospel singers bwanji? Mmmmm
mr Zamapemba,did u exhaust all options before seeking court address.You will scare away other would be supporting gospel artists becausse of your short temper attitude display.Do not overflood courts with petty issues like this one.
If I were the judge its the deposit plus interest. His failure to appear for the show has no bearing on why the gig was cancelled.
Nawe odala wayamba kuimba liti??? Ukufuna phiri akusegulire njira kuti anthu akuziwe mofulumira koma uzafuna,anakukana kukambirana nawe usanapite ku court ko??
Don’t be arrogant,he must pay everything that was spent
A zamapemba, kufuna kupanga profit from twenty eight thousand? Interesting!
Munthu osatchuka amadalira anthu wotchuka kale kuti adziwike ngakhale iyeyo James Phiri sadatchuke chifuka cha anzake kudzikonda bwanji? Muziyika Mulungu pa tsogolo
Wait a minute. If you are talking about gospel artists, I assume that you are talking about believers in Jesus Christ who have made this Jesus the saviour of their souls and Lord over all else they say and do. If this is true, then taking each other to a civil court is contrary to scripture which sets the standard for their conduct. It is unchristian, regardless of who was wrong and how much loss the offended has incurred. In everything give thanks to God. Let the world know your perseverance. The Lord is at hand.
As agospel singer u need to show gud mothers aPhiri chilungamo ndichofunika osamadyera dzina la Mulungu mukapsa ndithu