Email a copy of 'Malawi govt rejects Afrobarometer survey on governance front:  ‘Poverty levels extreme ‘' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

7 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
Real patriot
Real patriot
6 years ago

What can u expect from dunderheads like Dausi?He earns a living by concoting lies to defend the failed party.For your information this guy used to be a gatekeeper during kamuzu times.The robes are too big for this job.Zamukulira. Politics favours mbutuma most of the time because smart people do not like to be pushed by some failed visionless politicians.

Mudzamva liti
Mudzamva liti
6 years ago

Iwe be humane, tanthauzo la mau oti “Overall” umalidziwa? I think you don’t because if you do, you wouldn’t be asking for “gulu la anthu omwe mumawafunsa ……”. Stupid. Dausi, kuopa Mulungu ndiye chiyambi cha nzeru. Ngati iwe ndi anzako amene muli m’bomanu simuopa Mulungu, mudzapitilira kukhala opanda nzeru zoyendetsera boma lanu loipali. Zoona unganene kuti “the gap between the poor and the rich is narrowing.”? Abale ako onse kwanu ku Mwanza ukuwaganizira? Umatamba kapena? Pemene munthu ubvomereza kudzudzulidwa ndipamene umatha kukonzo zolakwa zako. Apa zikuonekeratu kuti this dpp government will never change and the only change will have to… Read more »

Rift Valley
Rift Valley
6 years ago

Dausi will never respond positively to anything to do with DPP’s poor performance when others would view negative survey results as a wake up call, an opportunity to correct things. Dausi’s main preoccupation is to please APM

Well, ignore wise advice at your own peril. It’s not only Afro barometer. Others have highlighted similar shortfalls.

Alinafe Phiri
Alinafe Phiri
6 years ago

Dausi akulakhula ngati mphwake was Satana amene amakondwera anthu akamavutika,moti momwe a Malawi akuvutikira angamanene kuti gap ikuchepa pakati pa osauka ndi olemera.Ufiti chiyani,Kodi saopa Mulungu akamalakhula mwachibwana moseweretsa miyoyo ya anthu.Pali aziphuzitsi amene adamaliza course yawo koma akungokhala,muzipatala mankhwala mulibe,Chanco ikukanuka kutsekula mpaka pano.
Tiyeni tizibvomereza kulephera kwathu ndikumulora Mulungu atipatse nzeru.

Bt@gmail.com
6 years ago

Yes the gap between the poor Dausi and the Rich is Narrowing. Not malawians!

CHIMVQ
CHIMVQ
6 years ago

YOU HAVE STARTED REJECTING THE AFROBAROMER RESULTS

MY KWESIONZ #
WILL YOU ACCEPT A BIG LOSS AFTER ELECTIONS WHICH IS COMING YOUR WAY AFTER ALL THESE BLANDERS YOU ARE
MAKING ??

GET READY OOOOOOOOOOO !!

be humane
be humane
6 years ago

nine out of ten is 90% not 88 percent. simple mathematics you mean mtolankhani iwe wa Nyasatimes masamu ngati awa ndi ovuta? Anthu mumapanga ma survey inu mudzitiuzanso gulu la anthu omwe mumawafunsa chifukwa pali gulu lina olo mulifunse answer timayidziwa kale. For example asking the opposition (power hungry parties) and the so called CSOs (money hungry organizations) about governemnt performance will rate it almost zero. Ask University of Malawi students will rate the government almost zero because of its failure to run the Tertiary education system. Then ask the malata and cement subsidy beneficiaries will give this government 95%.… Read more »

Read previous post:
Wizards caution over Mulanje Park usage

Premier Bet Wizzard have expressed concern over usage of Mulanje Park by other teams following a ground crisis that has...

Close