Email a copy of 'Malawi maize crisis worsening: Woman faints queueing on empty stomach' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

29 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
TA Teputepu
8 years ago

Munasankha nokha chimanga 4, lero njala yalowa dziko. Mumati chikukwanani bwanji.

Billy Chilewani
Billy Chilewani
8 years ago

It is a shame for my country year in year out to be hearing of hunger in the months of Dec-Feb each and every year. This last season understandable but the pattern has been there time immemorial. Can’t we for once both opposition ( which is Govt. in waiting) and the ruling who are supposed to map-a strategic direction for once come to the root causes of this perrennial hunger and root it out.Is it overpopulation as alluded to by Akweni? You may hate her but at the rate we are going,I think it is high time we shoulder responsibility… Read more »

Mngoni weni weni
Mngoni weni weni
8 years ago

Vuto laboma la DPP ndi tsankho. Kummwera makamaka ku Thyolo ndi Chiradzulo mwapereka zimakuponi zambirimbiri. Maka ku Thyolo poti ndikwa president komanso nduna yazamalimidwe. Pano fertilizer akuchita kutsala yet kwina kulibe. Olo chimanga kukumabwera zima truck daily. Pomwe ma ambulance ndimankhwala a kusowa mzipatala zina, imeneyo sinkhani ku Thyolo,. Ichi ndichimodzi mwazipatala zomwe zili ndima ambulance wochulukitsitsa, osatiso okufa koma woyenda. Koma pitani ku kasungu mukapeza 2 ambulances. Mankhwala ndikutapa kutaya yet kwina olo panado kulibe. Ndunena izi ndi umboni. A president ndi nduna zanu, can you treat all Malawians equally please. Boma la DPP linayambitsa quarter system yamaphunziro ati… Read more »

Sailota
Sailota
8 years ago

I am short of comment. Otherwise, let me condole all those that are suffering. Kodi chimanga chomwe tikuuzidwa, tinauzidwapo kuti bola lagula, ndipo ndi chokwanila chili kuti. Are u sure u were busy campaigning to illtreat your fellow Malawians? Think twice and act. Remember God is watching!!!!!!!!!

kaliyati
kaliyati
8 years ago

Sitidya loko timadya chimanga!! Sitidya loko timadya chimanga!! Sitidya loko timadya chimanga!! Sitidya loko timadya chimanga!! Uko kunali kuimba kwa Ana asukulu otumidwa ndi amphunzitsi masiku awo. Tilape amalawi ponena kuti Chipani china chimabweretsa chimanga. Malawi imadalira mvula ndipo mvula imachoka kwa mwini namalenga.

Burauni Mpinganjire
Burauni Mpinganjire
8 years ago

Malawi president – vakusi vanu.
Malawi cabinet – dull.
Malawi opposition – stupid & useless.

We told you here in September last year to find and despatch tractors to Malawi’s major dambos all along the lakeshore, to help local people clear land so they could plant dry season maize on a large scale. That could have helped mitigate the hunger situation by now. But there you were, busy flying to USA with large entourages with other people’s wives.

Ndiye ndi izotu wanthu ayamba kufa uko. Muthana nazo nokha.

All4ks
All4ks
8 years ago

Yet this stupid clueless govt all along was saying we have plenty of maize.

Jappie and msaka, dpp politicising maize by instructing their ministers or MPs to obtain maize through the Admarc back door and distributing to their areas. Buying votes for 2019. No shame these dpp dogs, people are dying.

Starling Kondowe from Chikwina CDSS in Nkhatabay
Starling Kondowe from Chikwina CDSS in Nkhatabay
8 years ago

The problem is,some of us are deepening the thorn of hunger in
most malawians.Maize in admarc markets is sold to vendors who in turn sell the staple food to the hungry masses at high prices.As we write,ferlizer subsidy is being sold at 15000 per bag.What are doing,as malawian? Let us do away with these evil acts and change the face of our nation.Together we can dimish hunger,Together we can phase out the so called neocolonialism,yes! Together we can build a better Malawi .

Dada Kampingo Jere
Dada Kampingo Jere
8 years ago

Makuponi mwapereka ambiri kumwera, koma dziwani kuti kumwera njala ndikumenenso imatidzimila kwambiri. North and Central mumatimana makuponi, ndiye Chauta pankhani ya mvula amatikonda

Violet Zulu
8 years ago

Mmmh this all because of vendors as well as admarc personells

Read previous post:
Joseph Kamwendo hunting for new club

Former Mighty Be Forward Wanderers midfield wizard Joseph Kamwendo has said he is hunting for a new club. The ingenious...

Close