Email a copy of 'Malawi parliament suspended over MPs demand for loans' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

22 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
Gogodasi
7 years ago

These guys must start paying tax and let them feel how it pains. Another thing is that the President should extend an olive branch to those MPs willing to return to Parliament to continue deliberations and leave out the selfish ones or else he can use his executive powers to dismiss Parliament and reopen it within a week and let those that have returned to pass the budget. I am 100% sure if he intervenes in this manner three quarters of the MPs will return including leader of opposition. Chakwera will have no choice, but to reason with his MPs… Read more »

Cash Gate
7 years ago

Vuto lilipo ndi carbinet yathu yomwe ikutenga ndalama zambiri, aphunguwa akudziwa zomwe zikuchitika ndi nduna zathu pamodzi ndi presdent podzikundikila ndalama zambiri. Aphungu chomwe akufuna ndi ngongole basi osati awapatse mawonjezero. Dziwani kuti abomawa alibe chidwi chotukula dziko lino koma kumangokhutisa mimba zawo. Carbnet yathu ikanadzipatsa ndalama zochepelako, nkhaniyi siyikanabwera. chatsalatu apa ndikumangokanganilana misonkho yathu basi osati kutaya nthawi pa nkhani za chitukuko. Bwanji osatisunthirako ‘ tax free’ kuchoka pa k20,000 paja kuti mwina kandalama katha kumatsalirako mthumba. Dziwaninso kuti tikapita kogula zinthu timakumananso ndi ma ‘tax’ okweranso mma shop omwe amawatcha ‘value added tax’ Chonde timvereni chisoni ife anthu… Read more »

Mfana odzisata
Mfana odzisata
7 years ago
Reply to  Cash Gate

I agree with you 100%. A Chaponda asaname its us who will suffer koma iyeyo ndi anzake.

Mulolopwa
Mulolopwa
7 years ago

In this case the MPs are justified. Chaponda should not fool Malawians in the name of buying maize when He has already pocketed from the ministry. We all work for money. The MPs demand is part of their conditions of service which all of us equally demand in our respective work places. To be an MP is not a voluntary job, its a paying one that comes with all Those conditions like loans that have to be honoured. If the ministers got theirs, Why not the MPs? And to My fellow Malawians, Lets not be taken for granted Because We… Read more »

Issa
Issa
7 years ago

aliyense wamboma tools down.

njoloti
njoloti
7 years ago

After 23 years of multiparty system of government in this country, iam convinced beyond doubt that as long as this system continues, no meaningful development will ever take place in Malawi.Fellow Malawians, you can see what these rogues masquerading as MPs are doing-literally holding the entire nation to ransom for their own selfish reasons.Malawians we need to go back to the drawing board to come up with a system of government that would cater for the needs of the people of this country.

The true Malawian
The true Malawian
7 years ago

Malawian MPs just know that you are digging your own political graves.The people of this country will never be taken for a ride by hyenas in goats skin.Come the year 2019 the majority of you will weep and wet your pats.Mark my words.

spectator
spectator
7 years ago

Ma MP adabwa nduna ndi a president atagawana papakulu iwo akupemba ka K3M ndiye muziti ndi adyera. Akulu akulu ngati Goodle ndi Chaponda akamagwirabe ntchito mmalo mochita retire achinyamata sitikhala ndi sogola pa Malawi pano ntheradi ndithu.

Douglas Ndindi
Douglas Ndindi
7 years ago

When campaign time for the next elections comes, I hope Malawians will remember that most of our MPs are there to represent themselves and not their constituents. Ndiye poti monga Atcheya Che Bakili Muluzi ananena, aMalawi tiri ndi vuto limodzi – sitichedwa kuyiwala. Why wake up very early on polling day to go and vote for someone who doesn’t care what happens to you thereafter? Wake up Malawians! We can put the time we spend on that queue to better use! Ndanenatu.

chitmukulu
chitmukulu
7 years ago

MPS ARE NOT GREEDY. THE MINISTER AKHUTA KALE . ZAWO ATENGA KALE LER AFUNA APUSITSE ANZAWO. HYPOCRITES.

Ma MP a DPP ali mkati momo kusapota adjurnment.. Ndiye wina akuti a DPP akuchitabwino

Gogodasi
7 years ago

Kalindo yenda maliseche anzako abwerere ku nyumba ya malamulo. Waziyamba, limba.

Read previous post:
Karonga Stadium on track for completion

Authorities at Karonga District Council insist construction work of the multi-million Karonga Community Stadium is in progress despite apparent lack...

Close