Email a copy of 'Malawi peaceful protests today: What you need to know' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Malawi peaceful protests today: What you need to know' to a friend
The Monjeza family of Katoto residential area in the city of Mzuzu had a thanks-giving mass on Saturday April 21...
amalawi azanga tikuvutikinji mulungu anatipatsa mnyamata amene alindi masomphenya amarifunila dziko lamalawi koma ndi anthu ake zabwino sakhala ndimbali or atampatsa ndalama zochuluka bwanji koma iyeyo anama pachilunga saopa koma amanena zokoza Malawi ndizothekatu amalawi tose kunena chimene chikufunika kuti dziko liyende bwino posankha fundo zabwino osati kumasekerela atsoreli akuba omwe akuvutitsa athu ambiri chifukwa akuika ndalama zoyendetsela boma mmatumba mwawoo ine ndimasapota sir lusius banda ndi kusabisa may kwa amalawi ose ndipo amalawi nose munakakhala ngati ine tikanangoti change nthawi imodzi paribe angatsutse gulu akadachokapo okha
Malamulo akulora ziwonetsero Peter Mutharika , Goodall ,Kondwani Nakhumwa ndi akatangale kwambiri aDPP agulukunyinda awo apanga zawo motsogozedwa ndi ng’ona zawo.
ndiye dzulo munali yaviyavi inu a diphiphi zazii basi abakha inu mumatikwana kwambiri
tikuti ma demo omwewo basi ndiufulu wawo
Why would DPP allow Public Order Police unleash unnecessary force on its own people. Why would DPP mobilize its unruly members to cause hard to its own people. Why would DPP not listen to its own people when they’re expressing their anger. DPP should learn to engage with the very people it is governing to be a better party.
The organizers need to share us their tweeter handles and whatsapp number – keep us on the loop
ma demo omwewo basi asamajaire
The organizers need to share us their tweeter handles and whatsapp so that are were kept in the loop
The organizers need to share us their tweeter handles, and whatsapp to keep us the loop