Email a copy of 'Malawi Police arrest 17 boys in local 'Boko Haram' gang' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

82 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
MAGEDE SIWANDALE
8 years ago

Comments are closed

musandifunse
musandifunse
8 years ago

14yr old acting as boko haram? Anena zambiri ana amenewo. The real boko Haram is coming

Nabetha
Nabetha
8 years ago

Asapite ku ndende but keep a very close eye on them.If they do it again then they deserve prison life. Nanga kuba phala tinganene kuti ndi mulandu woti mpaka ukanenedwe mukhoti? The issue here is not serious,they just need proffessional counselling. Dismantle this bad company rather.

Taona
Taona
8 years ago

This article is truly written by a foolish insensitive unprofessional writer. I say writer because to call them a journalist would be insulting to those who are journalists.

Boko haram is not a catchy term to be thrown around in titles to get views. Implying that boko haram are in Malawi is unprofessional, irresponsible, insensitive to real victims of boko haram and inciting unnecessary fear.

HE JOZA
8 years ago

Send them to mpemba boys home

Apo ayi alembeni ntchito ku utsilikaliko !!

akatswiri
akatswiri
8 years ago

writing on the wall

thomasstephano
thomasstephano
8 years ago

ndchan cheni cheni cikucitika dziko lapansi dis thngs its seens lyk dis is a past days bt kungoikiza mapemphelo dziko lathu lamalawi kt zimenezi zithe bas

pitala wachilomwe
pitala wachilomwe
8 years ago

ma gang ‘wo si Boko Haram,ndi Boma Haram

Blessings Adam Kaliapa

Vuto simakolo awo Ayi.Mwana amatha kuyamba zoterezi chifukwa cha azimnzake ocheza nawo.Monga mmene mwamvela nkhaniyi Panali ana ena a mchititidwe umenewu ndikale omwe amakakamiza amnzawo kuti awatsatile ku gulu lawoli.Koma ngati sakhala membala wagululi amapangidwa nkhanza chifukwa simembala wawo.Musawapake makolo awo apa.Kholo likhoza kukhala losamwa mowa pamene mwana wake amamwa.Chambachonso chimodzimodzi kholo osachidziwa Chambacho mwana mkuchisuta.

saziwi wankulu
saziwi wankulu
8 years ago

vuto sianawo koma makolo awo.mwana wazaka 14 akavute kumpanga handle.

Read previous post:
PVHO reforms under threat: Officers resisting change; suppliers not being paid

The Public Service Reforms which is being initiated by the Malawi government are being frustrated by the people who are...

Close