Email a copy of 'Malawi Police arrest Pakistan national, recover K19 million' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Malawi Police arrest Pakistan national, recover K19 million' to a friend
Second Deputy Speaker Clement Chiwaya angered lawmakers mostly from the opposition, over his way of handling the proceeding of the...
Malawi ndie ameneo sanganene kuti tapeza 23m koma ai tapeza zochepa zina tikufufunza mpaka zaka 4 kenako ithala momwemo……..
Kuchuluka amwenye nziko apunguleni Ku were azungu kaka ndi a nyaniwo
a Police amatengapo kumene, u think akapeza cash yo nde amakapeleka zonse? no wonder most of them are rich but without peace of mind chifukwa amene anabayo amakhala akuzunzika ku police iwowo akudya ndalama zosakhetsela thukuta. Atengapo 4 million imeneyo aaa.
Why are they found in Malawi??What has Pakistan done for Malawi??please kick them out of Malawi as soon as possible before it’s too late!!
Alot of pakis are living in Malawi without papers.The next thing you hear them,they have lost the passports and later on connive with the crooked immigration officers.Foreign investor from Karachi?Rotten Malawi.
bola apolisiwo nawonso asakhale atapeza 23mita yonse, iwowo nkumatulapo, kusiya 19 ikunenedwayo
Well trained mbava,cash gate inanso
Chori kartahai
Binchodi
Mase poes
Nayi
the suspect has been discharged by the court. The complainant changed statements in court that he has forgiven him coz of ramadhan. The magistrate went on to discharge him.
Katangale wayendapo ndithu!
Ndiye muziti kuMalawi kuli njala. A Mozambican planning to buy all that food from Malawi. If prices were well regulated govt could have benefited in tax and forex