Email a copy of 'Malawi police impound vehicle containing subsidized fertilizer' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Malawi police impound vehicle containing subsidized fertilizer' to a friend
Football Association of Malawi (FAM) haS sent to CAF Big Bullets’ application to participate in the 19th edition of the...
Stupid police mukusiya anthu amene akuba ndalama zaboma ma billion koma kugwira munthu ali ndi 3 bags ya fertilizer kusowa zochita chan
FERT SUBSIDI=POLITICAL,PLEASE STOP SUBSIDY NOW.THIS SHUD B LAST YEAR
Koma Phalula yomwe ndikuidziwa ine,aaaaaa nkulu uyu amaumira kupereka ndalama,pali ma offier’s achangu ozifuna ndiye kuti ndiomira ameneyo Kapena tinene kuti sanakumane ndi ajawa
feteleza mwagwilayo alindi chidindo choti ndiwa subsidy? Ngati alibe ingolekani poti mkapita kukhoti akadye yapamwamba ndi a khoti. Zilibe umboni kut ngwa subsidy. p
Kuba sikuzatha pa Nyasaland,wakula ndi umphawi
MTUMBUKANSO NDINDANI PAMALAWI PANO OSAPANGA BOMA LANU BWANJI ANTHU AKUBA INU MA OFFICE NGATI AKUGWA SIINU MA COMPANY ONSE AKUGWAWA SI ATUMBUKA NANGA MUTALOWA M’BOMA NG’OOOOOOO SIMUDZALOWAMO
A arthor mtambo tanenani zomveka sitikumvapo kanthu apa.
Thats why timati akhale universal subsidy mwaziona tsopano
Government is busy subsidizing business people on fertilizer. After a bumper harvest, the maize is exported to neighbouring countries in the name of trade liberalization. Malawian households left with food insecurity
wawa ife mavuto saztichoka zabwino mukupereka ku Mazambiki inu muzatengako chani