Apasidwe chilango chonkwima amenewo kuti wena atengelepo phunzilo.
NYAMBAMBA
9 years ago
My Malawi where are we going? Is this the same Malawi a GOD fearing country?? chadza ndi yani thupi la anzathu kukhala popezera ndalama.let us join hands and pray hard for deliverance of our nation .These albino have also a right to live same as normal human beings imagine aliwanu .Mkwiyo wa Mulungu ukukanthani soon.
Namalira
9 years ago
Tithetse asing’anga onse chifukwa ndiwo akumanamiza anthu Kuti alemera ndi ziwalo za alibino. God will punish all asing’anga abodzawa.
Kulibe kantu
9 years ago
People from Southern Region? Kukonda ndalama. Plz send this guy to jail immediately.
iman
9 years ago
Are these kidnappers people with all senses?ee anthu kumachita kuzinga ngati nkhuku kuti apeze ziwalo? Eeeish kuopsa dzikoli!!!
These kidnappers whenever should just be given death sentence, eye for an eye.
MENYANI CHITSILU KUTI OPUSA ATENGELEPO NZERU
OSAMUSIYA AMENEYU AULULE AZAKE ONSE OPANGA
ZOPUSAZO
life imprisonment for that stupid idiot. uchawa eti
Apasidwe chilango chonkwima amenewo kuti wena atengelepo phunzilo.
My Malawi where are we going? Is this the same Malawi a GOD fearing country?? chadza ndi yani thupi la anzathu kukhala popezera ndalama.let us join hands and pray hard for deliverance of our nation .These albino have also a right to live same as normal human beings imagine aliwanu .Mkwiyo wa Mulungu ukukanthani soon.
Tithetse asing’anga onse chifukwa ndiwo akumanamiza anthu Kuti alemera ndi ziwalo za alibino. God will punish all asing’anga abodzawa.
People from Southern Region? Kukonda ndalama. Plz send this guy to jail immediately.
Are these kidnappers people with all senses?ee anthu kumachita kuzinga ngati nkhuku kuti apeze ziwalo? Eeeish kuopsa dzikoli!!!
Anyamata kufuna kulemera nsanga mwagwanayo school munathawa kalekale munya muona mxiiiiiiiii!
Let Them Be Slapped By Justice