Email a copy of 'Malawi Police officer convicted over illegal possession of charcoal' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Malawi Police officer convicted over illegal possession of charcoal' to a friend
Over 100 football supporters have won different prizes in ongoing in the ongoing Zampira promotion. Launched on June 7, 2017,...
Galimoto mupatseni makala ndi Galimoto sizikugwilizana ayi .Anthu akuba zinthu zinthu osati makala ai wakabela NDANI makalawo. Simwati ndimitengo ya chilengedwe ndiye kuti siyamunthu ndiyamulungu mumveleni chisoni
Galimoto mumupase munthu sizikugwirizane ngati zili mumalamulo chosanimoni chifukwa makala ndi Galimoto ndi zinthu ziwiri zosiyana ndipo sizizafanana mpaka kakle kale!
they have started selling charcoal because of poor economic in Malawi, they failed to pay school fees for their children due to low minimum wage in Malawi, instead to prevent they start destroying. zonsekensa bwanji a Malawi
asalanso ena ofunika muwagwire alipo ambiri mu Police college ,they use their work as a tool some are also selling chamba
The Hunter has become the hunted…
Koma George Chaponda wangosiyidwa kumamwa vinyo ali phee pamodzi ndo Goodall and Peter Mutharika.
Law enforcement at its best! The question is, who is policing who? Who is hiding from who? Who are the criminals between civilians and the men and women in uniform? Koma ndiye abwana mpaka muluze Pajero chifukwa cha makala? It’s true that this world is round, and everything in it goes round and round.
Inu iweruza ndichifukwa chiyani akufika pogulitsa makala?