Email a copy of 'Malawi Police re-arrest Dauka Manondo on alleged plot 'to kill witnesses'' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

48 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
Shonayi
8 years ago

Atumbuka ndiye mwayalatu.Anzanu amatukul kwawo nanga inu osakatukula kwanu bwanji

Hoitty
Hoitty
8 years ago
Reply to  Shonayi

I hope inu kwanu munatukulako ndipo kwanuko ndiku Lilongwe city kapena Blantyre city osati ku Blantyr or Lilongwe rural poti mkosauka momvetsa tsemwe. Ngati kwanu sikuma city awiriwa koma ku ma boma ena katukulenikoni chifukwa nkosalira. Anthu mmalimbikira ati kwathu mku Blantyre chonsecho kumudzi kwanu ku Neno kaya Thekerani palibe chilipo. Mudzitamika ngati kwanu kuli kwa Kaliyeka kapena ku Chileka. zoona ine wa ku Nsipe ndidzinamize kuti kwathu nkotukuka kumanena Lilongwe??? kuganiza mopelewera

Mwenecho wa sima
Mwenecho wa sima
8 years ago
Reply to  Shonayi

Munthu uzichokera kwa ngwangwa kaya ku simuchimba ndikumanena kuti kwathu kotukukuka?Mwa achina mbayanii kaya mwagoliyo mu ndirande umu amaba. Nsima ilipamoto?Dont waste time Kulimbana ndi mtundu wozindikira ngati atumbuka.

Gorbachev
8 years ago

Why this issue is taking so long

Shonayi
8 years ago

Amayi Banda ndi mfiti yeni yeni.Moti ana amene mumkawatuma mungawakanire poyerayera chomcho.Akubvutikatu mukuona.

elton banda
elton banda
8 years ago

we gettin tired with this cash gate issue, mwatikwana ndi zopepela zanuzo, kodi and amenewa atipindulira chani ife anthu osauka?

chejali
chejali
8 years ago

Kayaa no coment pa izi

Nachanje
8 years ago

mukuchedwesa chigamulo mvuto lake

Felix Kajawo
Felix Kajawo
8 years ago

Let The Law Act Accordingly,These Guys Are A Threat To The Nation

Maravi Peoples
Maravi Peoples
8 years ago

Anangotengeratu ntchito zonse za satana Kuba Kupha ndikuononga ana a Manondo bwanji?tinene kuti ndi ntchito yomwe ya manja munatengera kwa atate anu chifukwa sizitheka ana m banja kupanga makhalidwe oipa lofanana

Kanda
Kanda
8 years ago

Inu zoona kufuna kuphaso wina aaaaa ndinu ovutadi eti kaloweni.

OGO!!
OGO!!
8 years ago

It is utter wrong that these individuals who have personal issues were used by the people in power by targeting their vulnerability and problems to achieve what they wanted. And now that things are not as rosy, these small fish are being tossed around like this. I feel the justice system in Malawi is wrong. Why not get the big fish rather than overlooking the acts of those big fishes…? It is unfair but as the saying goes…if you are a nobody in society, you have no where to go for support. Its unfortunate that the Manondo brothers were linked… Read more »

Read previous post:
Airtel beefs up security for Lilongwe TTC demonstration school

Headteacher for Lilongwe TTC Demonstration School Caroline Majiga has applauded Airtel Malawi for the timely donation equipment that will enhance...

Close