Email a copy of 'Malawi protests over food  shortage, economic woes March 10' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

33 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
HPB
HPB
8 years ago

Nyasatimes does a good job of reporting the challenges faced by the country. The on-line publication also articulates the views of the opposition very well.

But the coverage does not provide responses from Government. This is unsatisfactory. For example, what is Govt’s response to the food distribution problem? Can we, please, have news of specific areas like what was done in Karonga.

I am not defending anybody; all I am looking for is balanced reporting so that readers are aware of both sides of a particular issue.

Game out!
Game out!
8 years ago

Kaya zanu izo. Ine kuno kwa a Kabudula dowe ndamuyamba. Ndipo tonse tagwirizana kuti 2019 Chakwera voti olo imodzi asadzaione chifukwa akuletsa nseu omwe Pitala akutimangira. Zimenezi ngakhale mafumu akudzidziwa chifukwa sizisiyana ndi ufiti. Tonse pamodzi ndi mafumu tagwirizana kuti mgalatiya ameneyu adzaidziwe Bangwe come 2019.

APM
APM
8 years ago

Mayaya ukunena zoona dziko landikanika. Naye saulosi ndimayesa amatha ntchito koma Nate zamuvuta. Airtel amkamuyendesela ndi amwenye aku India. Chakwela zandilandile udindo

Mytake
Mytake
8 years ago

All those opposing the demonstrations should know that holding peaceful demonstrations is a constitutionally guaranteed right. Secondly the Peter Mutharika DPP govt blundered by underestimating the maize required hence the scramble of maize at Admarc markets. It is the incompetence of the Executive arm of govt that has brought about the problem of shortage of maize.

magawagawa
magawagawa
8 years ago

a Mayaya, mavuto ali mdziko muno, sanabwele ndi Peter koma Joice pobetsa chuma chankhani nkhani, bwana wako Mayaya ndi Kamulepo. Iwe kabwila unakomela kuchoka ku CHACCO pano kuli ziii! maphuzilo akuyenda. Munthu oti chilichose chikhale cha NEGATIVE unabadwa bwabji? kunali anzako, Kalinde, Loveness Gondwe, Benison Linjenda ngakhalenso malemu Nga ntafu, amavuta ku Paliament koma lero kulibe samalani polankula tikukuonani kuno kumadela kwanu, osamalankhula zoti anthu azikutamani ayi chenjelani.

Phwitika
Phwitika
8 years ago

Some comments are DPP die hards masquerading as meager citizens here. Ingokhalani chete, akutumani ambuyani eti, matako anu!!!

Kadakwiza
Kadakwiza
8 years ago

Malawians don’t need to demonstrate but Malawians need revolution. I remember there was a protest before and what happened, did the government took steps I don’t think so. What we need in Malawi is revolution and force our present government to step down.

Boliwoli2
Boliwoli2
8 years ago

Mr.Mayaya ndikuvomereza zimene walemba vendor kuti ngati kungakhare ma demo achitike maboma onse not only ll as usaid.The whole Malawi kuli njala.Azingonyamuka kupita ku Thyolo mkulu uyu wativutisa.

vendor
vendor
8 years ago

but why only in LL. spread in all cities of Malawi. we are all hungry to get maize

mike
mike
8 years ago

a mayaya, muja munayambira ma demo chikusintha ndi chiyani? Osapeza china chochita bwanji,

Read previous post:
Spies scare puts opposition, govt on collision course in Malawi Parliament

A spy scare nearly put parliament to a standstill on Tuesday as opposition legislators wanted suspected spies from National Intelligence...

Close