Email a copy of 'Malawi public has lost trust in police, says IG Kanyama' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Malawi public has lost trust in police, says IG Kanyama' to a friend
Malawi civil society organizations (CSOs) have maintained that they will go ahead to stage a nationwide peaceful demonstration over the...
pa Malawi ngati kuli station pali a Police achinyengo ndiye ndi ku Mangochi Police.Mbava zokhazokha
(1)Pakhale special commission (Indipendent) 4 recruitment (2) Reduce Traffic police Officers on the roads and deploy them to various police Stations to help curb crime
The IG is stating the truth. If the police can rob and rape us then we are not safe and our trust on them is gone.
Munena zoona bwana a police enawa ndi akawalala, ndipo ntchito anayamba bcoz of ambwiyawo kapena ulova basi, ndiye akumapezeka nawo mgulu la mbala, achoke mutilembe ife a police enieni osati a kwakwase akuba amenewa. Achoke ngati ntchito atopa nayo ife mapolisi amwambo tigwira ntchito imeneyo iyaa!
abale nafe ana amunaperi takwiya ndi a OC apa soche mayiwa ndi uchitsilu kuyikira mbava kumbuyo amatero?
Very few polite men who admit failures, this officers dent police image due to their inborn behaviour
Bwana mwanenazo ndizona chifukwa ineyo ndi mmodzi amene ndilibe trust to any Police Offecer ali kuba kuposa MBAVA ZAFUTIM
Kanyama ndiwe mbuzi ziphuphu wayamba ndiwe abale ako okwa 50 ali ku recruit ndiye ukuganiza kuti anga gwire ntchito bwino?
simply saying people have lost trust in the police isn’t enough, we want action! In fact some of us lost trust in the police way back – from than 5 years ago. The killing of the poly student (Chasowa), thugs sharpening panga knives in broad day light in Blantyre, the list is endless.
where are we heading to?
These days when I see a policeman/woman, I fear for my life. I don’t know what will happen next…will he shoot at me? will he steal from me? will he beg from me?
At first we thought delays to reach the crime scene was because they had few vehicles but now its clear that they do it deliberately as they know some of them are among the gangs terrorising the country.Thanks Mr.I G that u have acknowledged our distrust in your pple.