Email a copy of 'Malawi public hospitals hit by electricity crisis - Nurses' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Malawi public hospitals hit by electricity crisis - Nurses' to a friend
Malawi national team and Mozambican based HBC Songo international goalkeeper Charles Swini is very doubtful whether he's going to be...
Lucius Banda wayimba nyimbo. Akutiwuza mwanthawizonse kuti ngati chinthu sichako sungachisamale. Pamene timamenyera ufulu wadziko ili enawa anali ndi magrini kadi-anali nzika zamayiko ena. Nzika za Malawi zikamadandaula iwo alibe nazo chidwi. Ana awo akukhala konko. Alibe ndichidwi chomwe kuti ababa ndi a president tipite kwathu ku Malawi, ayi chifukwa akudziwa kuti kulibe chabwino. Akaba ndalama apita nazo kwawo ku America.