Email a copy of 'Malawi Queens  star weds long-term partner' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

11 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
godobaman
godobaman
9 years ago

inu ndiye mwayitha chemwa mwapeza kasinkhu wanu ndithu osati a Tina anapeza nzungu okugwa ndikumina ati kufela ndalama munthu othaitha kale ameneuja shame on you TINA

Kulinda Mtere
Kulinda Mtere
9 years ago

Ayise Masa, washosha dala mwali wa fitness ya kathithitu. Nde nawenso ofunika uyambe gym. Nanga lobodolobo akuoneka mu jacket yo akuthandiza?

Samson
Samson
9 years ago

I find this to be in order!

Mbolo Sidwala
Mbolo Sidwala
9 years ago

Chitsanzo koma chimenechi, osati tinazimva last week! Anthu amalowa m’banja ali ndi mwana kale, munthu wa Mulungu nkumati mukhale chitsanzo kwa anzanu. Meaning what?

Chikopa
Chikopa
9 years ago

Zabwino zonse kumakondana osati kumenyana paja anyamata amasiku ano chamba

VULUNGANYA
9 years ago

Bolatu uyu osati aja anangotola mzungu wothayitha aja.

Quota system
Quota system
9 years ago

I seem to know the gentleman on the far right. He is a clinician. It was great indeed.

khwinda
khwinda
9 years ago

comgrats Bayano n Towera nzabwinotu izi mwachokera patali guys

mnchindo wa satana
mnchindo wa satana
9 years ago

Kaya zanu izo. Ife ndiye tili Ku lake of stars

chekambewa
9 years ago

Bwino mukasamalane osati muziti yaviyavi ndi vidya makanda vamatenda mumpake nyamatamata ngati ameneyo. thats good wakwakwaza kanyamatatu osamakomedwa ngi khusa ngati zinzzija

Read previous post:
Regionalism, tribalism tearing Malawi apart

Calls for secession, specifically for the Northern Region and federalism (preserve of the Central Region) are refusing to be silenced...

Close