Email a copy of 'Malawi VP Chilima make appeals for patrotism, population at Mua Parish celebrations' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Malawi VP Chilima make appeals for patrotism, population at Mua Parish celebrations' to a friend
Minister of Information and Communications Technology Nicholas Dausi eulogized veteran radio drama Smart Likhaya Mbewe Sunday as one of the great sons...
Kodi bwanji osangokhala mbusa Chilima? tayankhulanikoni zakuwotchedwa kwa anthu manja anu adeko pang’ono kumangokhalila mumipingo sizikuthandizani nthawi zina tizimvapo kuti mukukumba mjigo kuti anthu amwe madzi ku uliya. Nthawi zina tizimva kuti mwatseka gate ku Capital Hill kuti ma Civil Bosses obwera mochedwa asalowe, Nthawi zina tizimva kuti mwakayima pamzere ku Queens kuti muwone kuti anthu akuthandizidwa bwanji. Changamukani patown nthawi yatha.
Koma mpingo wake wokaniza makondomuwu ndiye musovenge. Muzingoberekapo basi. Primitive church. Aids simukuyiopanso – no to condoms?