Email a copy of 'Malawi women cops face abuses in homes, work places' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

23 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
Joseph Gowa
Joseph Gowa
7 years ago

Kuyelekedwa akazinu.Mamuna akayende kunja,nsanje thoo. Achite iwe wekha mtudzu mbwee. Mamunayo atanino? Rubbish

Major General
Major General
7 years ago

Osanama azimayiwa ndiokwiyadi mwina zimayambira ku training school kwawo ndiye ndi mtima okulawo amayamba kuchitilanso mwano azimuna awo. Munthu sungangoyamba kuzunza mkazi wako opanda chifukwa kapena wachambatu nanga munthu wabwino bwino. Palinso azimayi ena apolisi kukonda kuledzera ulowe pub iyi ali mommo upite iyo alikonko ndiye choncho zinthu zingakhale bwino. Komanso nkhaniyi si kupolisi kokha.

Akungolonje
Akungolonje
7 years ago

strawberyy juice,
Mai yo ndi wanzeru, adaona kut vuto udali iweyo komanso nkutheka kuti amakudziwa bwino lomwe kuti mwina khalidwe lako ndo lonyasa losalemekeza mamuna wakoyo. Mwinanso umakana kukuchinda kumachita ukudziwa kuti ndi mwamuna wako ndipo chakecho udalimbirira pa maso pa Mulungu wako kut ndi chawekhawekha basi. Tsono ngati umankana umati iye asakumenye, iye samafuna kukachinda ma hule a ku Bar ununkha fungo la kondomu akangovula, amafuna Iewyo mkazi wake monga mwa lonjezo lako loti ndi chawekha basi

Akungolonje
Akungolonje
7 years ago

Prince mpasakuphe,
I totally agree with you guy or girl. The police women are generally very rude. The always and everywhere want to be felt highly and knowledgeable. The have no respect with others as such they can and will not respect their husbands or family members. Police women are very cruel and inconsiderate to the general public. I have no grudges with them but simply saying the truth and reality. Too much mtudzu ndi mwano amayi apolisi even akazi a police (housewives) ndi chimodzimodzi khalidwe lawo. Akhala pagulu amafula akhale oyambirira pa chilichonse.

frank
frank
7 years ago

mkazi wa polisi ndi wapolisi basi si banja ayi

prince mpasakuphe
prince mpasakuphe
7 years ago

It is common knowledge that marriages in africa are founded largely on the basis of culture. Our cultural values and even the bible explictly stated that akazi inu mverani amuna anu. The challenge comes when the woman want to do policing in the house. In other words most of them fail to undress the police uniform when in homes. I personally dont think it is a question of rights but rather discipline

Winston Msowoya
Winston Msowoya
7 years ago

Candidly I have no grudge against Police women,but of course,generally,they behave impudently and irrespectifully in their places of work it is unusual to find a dignified and well mannered Police woman in Police Stations or offices.They have adopted very outlandish way of life that is beyond our culture,they look down upon their husbands especially those husbands with low income brackets.This habit seems it is worldwide,in Canada,women are .more powerful than their husbands and this many times has ended up in grave sequel.My advise is calm down and solve the dispute amicably otherwise you will end up into more troubles.In Malawi,this… Read more »

Mkoke
Mkoke
7 years ago

Iwe strawberry juice..tanena banja lakolo liri pati pano? Linatha monga? A polisi si a nkhoswe a mabanja. They r trained to decide when to intervene or not to. Atakufunsani mafunso awiri atatu anafziwa kuti mukufuna kukhalabe ndi amunanu. Now i know kuti u r failing to resist the urge of lying to us that u divorced…just saying

Chithumwa
7 years ago

Ndani wamisalayo angakwatire mkazi wa POLICE? Mahule? Angakhale ndi banja la ulemu amanewa ? Kukula mtima, Akuti kudziwa malamulo, 4Ja basi.

Clement
Clement
7 years ago

Malawians let us change our mindset and start respecting our lady cops. Most of people abuse female officer just to test me. Bad manners

Read previous post:
Malawi govt approves K1mil loans for councillors

Government has approved loans for ward councillors who are now entitled to K1 million each. Spokesperson for the ministry of...

Close