MWAONONGANSO NDALAMA ZIJA, KUMATENGA ANTHU KUTALI AZIBAMBO, AZIMAI, ANYAMATA, ATSIKANA, NDI AMAKWAWA KUPITA KU BLANTYRE, OSATENGA AKU BLANTYRE KOKO, BASI KUFUNA KUBA NDALAMA KUZAMATI KUTI TINALIPILILA MAGALIMOTO, CHADYA NDI ZINA NDI ZINA ZA WANTHU OBWERA, NDI MALAWATSE MUKATI.
MWABA ZOCHULUKA ENA OVUTIKA ALIBE CHILICHOSE ——- HA TSOKA ILO
Chief
9 years ago
Kodi agalu inu, kumapepheloko msalu zachipani zimakataniko?komstu mudya michenga chaka chino.makamaka ku mwera kwa lomweko.mutong’ola chili pa msalucho.
it was only last month you went to pray to your god for rains, today you’re praying to him/her(especially catholics to mary) to stop the same rains, are you ok in your minds?? didn’t you ask your god for an amount of the rains at the first place?? there are floods, storms etc in America and all over the world, have you ever heard of Obama organising prayers to god?? for what?? this is waste of money, time and energy. the lost resources could have been used for more productive course, eg civic educating citizens on need to take care… Read more »
My understanding was that the prayers were convened to remember those that perished in the floods and not necessarily to pray for God’s intervention on the incessant rains. So before criticizing read and re-read.
MWAONONGANSO NDALAMA ZIJA, KUMATENGA ANTHU KUTALI AZIBAMBO, AZIMAI, ANYAMATA, ATSIKANA, NDI AMAKWAWA KUPITA KU BLANTYRE, OSATENGA AKU BLANTYRE KOKO, BASI KUFUNA KUBA NDALAMA KUZAMATI KUTI TINALIPILILA MAGALIMOTO, CHADYA NDI ZINA NDI ZINA ZA WANTHU OBWERA, NDI MALAWATSE MUKATI.
MWABA ZOCHULUKA ENA OVUTIKA ALIBE CHILICHOSE ——- HA TSOKA ILO
Kodi agalu inu, kumapepheloko msalu zachipani zimakataniko?komstu mudya michenga chaka chino.makamaka ku mwera kwa lomweko.mutong’ola chili pa msalucho.
Unity for the good purpose
Ovutika ndi owonela eni ake akuziwana
it was only last month you went to pray to your god for rains, today you’re praying to him/her(especially catholics to mary) to stop the same rains, are you ok in your minds?? didn’t you ask your god for an amount of the rains at the first place?? there are floods, storms etc in America and all over the world, have you ever heard of Obama organising prayers to god?? for what?? this is waste of money, time and energy. the lost resources could have been used for more productive course, eg civic educating citizens on need to take care… Read more »
My understanding was that the prayers were convened to remember those that perished in the floods and not necessarily to pray for God’s intervention on the incessant rains. So before criticizing read and re-read.
OChakwera odathawa pa guwa lansembe odasiya kupemphera.Pano angotsilira Apm.
Kikikikiki nthawi yonseyi anali kuti awa. anthu afa uko mukubwera pano. Kutoleranso ka meagre 600 kwacha, kachani?
Next time osazawasiya asilamu kupemphelera mvuala ayi, mwaonatu, mvula yake ikumabwera ya boko haram.
Does this mean UDF never participated the event yo!signs and symptoms when the party is going to die no wonder,See MY Name Name.
Bambo tonde wadula simumadziwa kuti UDF inamezedwa ndi DPP? Ifetu tinadziwa kale komano kuti mumufunse Atupele ndi anzakw omwe akudya nawo za DPP akuuzani kuti izi UDF idakalipo adzakuuzani choncho chifukwa iwonso sakudziwa komano atsekuka mask kutsogolo kuno nambala ya aphungu 14 yomwe anawina ija ikafika pa atatu.
APM umakhwana, apastseni moni mbusa otembeleledwayu!!
Take is easy. Dont judge him too early. He may laugh last.