Email a copy of 'MBC fires Mungomo: Board finds him guilty over theft and forgery charges' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'MBC fires Mungomo: Board finds him guilty over theft and forgery charges' to a friend
The Brown Political Review (BPR) had an exclusive interview with Dr. Joyce Banda who served as the first female president...
uyu mukuti Albert. Kuba anayambadi kalekale gologolo wachabe chabe. Mkuluwakenso Brian chimodzimodzi. Albert saziwa ntchito ta pang’ono amabisalira kwa anthu andale to protect him. MBC muyang’ane ma voucher akale you will find kuti ma trip a Albert ambiri anali a Fake. Tsiku lina ndinakumana naye mu corridor ku ntchito kuni akuti I’m chasing my cheque I have a trip to Lilongwe Ati ku meeting. Mbava yachabe chabe. pano pa MBC Ku Administration yathu pofunika Kusintha amangosainira zilizonse without veryfying. Ndalama zambiri zimatuluka chifukwa cha weak administration. UYU Simango yamukulira ntchito. Komatu Albert apite kuchitokosi.Finance yathunso is so weak. Staff must… Read more »
Koma kankhopeko kutuwa chonchi ngati kuti wazola sopo ya Maluwa kumaso? Kodi sangathe kugula ka Vaseline or ka Cocoa butter ndi ndalama zokubazo?
Going to Mangochi just to attend to a thief? The chairman of the board needs to be fired…if only Mutharika was like magafuli or any other president who understand the dire situation malawi is in…i cry for this generation they have rotten wrong models in leadership position
I have met Gloria and she has confided in me that she is regretting leaving her loving husband Ralph for Mungomo who lured her with stolen money.
Gloria waneneratu kuti mmene zilirimu adzingonyengetsa to maintain her life style!
Musalimbane ndi ine. I am not your size. I am well connected. Do not waste your tome talking no sense. I will soon be back and i will be back with a a bang.
Mumalembelanji ntchito mbavayo mukudziwa kale mbiri yake? Zisathele pompo izi koma imangidwe basi.
a mungomo. chiwandatu chimenecho. mudzipempherere
Zamanyazi izi. Mpakana forging ma signature a anthu? Mlandu winansotu uwu. Chonchobe.. Koma asakalowe mchitokosi thanzi lawo will be compromised
Mummangise minty woipa ameneyi.Like sukulu alibe alowera kuti? Kukula konseko no first degree no wonder amabisalira my ndale.June mungomo anayamba kalekale.If you check me help ambiri amene wayenda that were fair like amagwirizana bro Mr Simango ku musainira ndikugawana zina.Achita zambiritu anyamata amenewa.
Welcome to Malawi where you can be fired from your government position for stealing the peoples money, then to be rehired into the same government department and do it again
Hopefully this will be the last that we see Mungomo
Sadly not likely
This guy looks like a habitual and con thief……..
No wonder the govt is full of thieves.