Email a copy of 'Mbendera says JB’s move on Malawi polls amounted to a coup' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Mbendera says JB’s move on Malawi polls amounted to a coup' to a friend
Flames technical panel through the Football Association of Malawi (FAM) on Wednesday 1st October, 2014 announced names of foreign based...
Iwe maxon wasowa chopangira mkomia kwa kahuna eti? Usatinyase
Kulumburitsa president mu khoti. Sizidawonekenso. Zaukhruku basi.
Mbendera wasowa nkhani. Asatinyasepo apa! Mbava yachabechabe. Akulephera kulipira anthu ena omwe adayendesa chisankho cha pa May,20. Why is he diverting our attention to his mumbo-jumbo talk? Muwapase anthu ndalama zao. Anthu amenewo adabesa tulo tsiku limene lija. Koma ndithu Mbendera osawamvera anzako chisoni? Muwaberenso akuzavotetsa pa 7 october wo, mutchuke ndiiiinu!
Mbendera atsamayakhure zimenezi pano .Ma elections onse anawonongeka chifukwa cha iye,sono pano asamakambe za nthobwa chifukwa zonse zadutsa.Ankalekeranji kunena nthawi yomwe ija?Mbendera tangotulani Udindo apa and mutsakakamire pampando pamene anthu anakupangani DISAPPROVE kale.Zinthuzi ndizotsiyirana sono STEP-DOWN others should continue with the good work.Usapangitse kuti DPP imange Joyce Banda chifukwa cha mabodza ako ukubwebwetawo.No one can believe now after four months since 20May elections.
Mbendera messed up big time, there was chaos in Ndirande and other parts of the country because Mbendera handled the polls very incompetely, after coming to his senses and fearing that violence might engulf Malawi because his own incompetence he asked Odillo to assist in security matters, this was even available on live tv and radio, he must instead be thanking Odillo and MDF for their services to MEC and Malawi. Those tears were they genuine. Mbendela Achoke! Achoke! Achoke!!!
MAN NDIZABODZA
big up mbendera
Ife a chipani cha pp tikuti zisakho zinayenda bho and peter akuyitha bravo Mec and DPP .
Mbendera shld not be trusted, he is speaking out today nusty things about amama bcz she is not in control. Mr Mbendera failed to handle the elections, he shld not clean himself up here. Analira powulutsa zotsatila za chisankho chija and lero akufuna azioneka ngati ndiochenjera, angatiuze chani. Chisankho chimene chija chinali ndi zolakwika zambiri, iyeyo Mbenderayo amadziwa kuti he is giving Malawians wrong results and thats why he cried. Ngati mwalandira ndalama kuti lero muime pachulu nkumalalata, a Mbendera, mudziwe kuti Mulungu akukuonani and achita nanu. Lino ndi dziko ndipo zinthu zimasintha, PP can bounce back in 2019, if… Read more »
koma xikuoneka muocha msumboni onse….ndipo a bwana mbendera….mwaonekadi crocodle tesrs…. mwafumbata kanthu ndipo tawona.
moti mafuna federsllusm &refredum… koma mukhale mtavhoka….resigm mwene!