Bola MCP not anamaujeni a DPP agalu akuba. Even Chilima says we must not elects mediocre leaders such as those in DPP. Chilima is tired of APM. Of course Chilima is himself not a leadership material but at least he has admitted that APM and his crooks are useless.
May his soul R I P.
Munya muwona, pofika 2019 azimwalira ngati ngumbi asakwi amenewa
Pepani a kubanja lofedwa, pepani a Speaker, pepani banja lonse la MCP. Mzimu wa a Jiya uwutse mu mtendere.
Mmmmm
I we mwinithako ndiwe chitsilu galu. Zikugwirizana bwanji IFA ya Honorable Jiya ndi ulamuliro wa MCP. Abale ma comment enawa tamaikani moganizila.
Kodi A congoress amafanso
Safa koma amwamwalira
mfunso lopusa
mukuyamikila imfa kapena mukuyoza munthu omwalila,pofuna kupeleka ndemanga pa imfa chonde umunthu ukhalepo no matter saliwachipani chanu chifukwa mawa ndinu kwake kwapita R.I.P
Very Sorry The Biggest Party!A You Are Loosing Important People. Lets His Soul Rest In Peace.
MHSRIP
MCP chingakhale Chipaninso choti chitilamulire aMalawi???Kungoawona a Jiya kokha kudziwilatu kuti inali nkhondo ya Young pioneer basi!!Mmene anali MYP chief sikumenya kwake makofi mbambo uyu!!!@
Mawa ndiwe. Just wait!
Bola MCP not anamaujeni a DPP agalu akuba. Even Chilima says we must not elects mediocre leaders such as those in DPP. Chilima is tired of APM. Of course Chilima is himself not a leadership material but at least he has admitted that APM and his crooks are useless.
Monga Dausi