Email a copy of 'MCP 'rebel' leader Chatinkha claims getting death threats' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'MCP 'rebel' leader Chatinkha claims getting death threats' to a friend
Malawi is likely to face financial penalties of up to K8 million for pulling out of the 2019 Africa Cup...
A Chatinkha, musavutike ndi kufufuza. Amene akufuna kukuphani ndi omwe anapha a Gadama, a Matenje, a Sangala ndi a Chiwanga.
anthu akuphawa, ndi oipa mtima regardless of their church background.
Chokha chongobwera pa MBC,zonse zidaonogeka pa umoyo wandale.Mwina kapena mungoyesa DPP yomweyo.
Chatinkha, wadya zambiri za DPP koma walephera kukwaniritsa zomwe anakutuma a DPP and no they will be on your neck so that you pay back their money. They are the ones giving you death threats. DPP imapha mayi, ukapanda kuwabezera zawo akuchinda ndi Mpeni ma Cadet a DPP. Udaziyamba wekha ndipo uyembekezere kuchindidwa ndi mipeni ndi zikwanje.
koma ndr kusakwanitsidwa, kwa AMERICA munakhala mwa ofuofu under our parents tax. osangoleka bwanji muti muphe azimuna a eni ake ndi matanda. decades and decades mukudya za boma . greedy pipo.
koamatu sibwino. msiyeni mzimayi. mukamatero ndiye kuti wakukanani kuti mumuchinde basi muthane naye politically azibambo muli ndikanthu. Jessie anakana kumuchinda basi munamuchotsa.uyunso chimodzimodzi. women empowerment yakanika basi
mmmmm amayi awa ndi kathyali, dyera komanso ndi madzi amene satha kupanga chiganizo paokh,amangolondola kumene kwaloza khwawa.
Death threats is not the hallmark of MCP but the same DPP whom she is helping. Yalephereka deal wakanika kupanga ganyu ndiye basitu zakuvuta. Ulipira bwanji ma million anakupatsa aja?
Chatuinkha is saying that as a pretext to find a way of returning to the MCP fold because she has realised that she was fooled by the thieves. Mlongo, just follow the footsteps of Mulomo otherwise if you continue aligning yourself with the thieves, you will never achieve your political ambition, they will just use you like Nakoma . This is free advise. I will rule Gambia for a billion years.
Madets amzake ndiapemene akumuopyeza. Wadya zambiri za DPP. Simunagwane moyenela.
I support Chatinkha’s game changing attitude, this woman has class, aptitude and ability to think outside the box, She is not your ordinary person. You go where mos tof us dont dare! YOLO! ( You only live Once! ) And you have chosen to make the most of it!