Email a copy of 'MCP says Malawians best judges on who between Mutharika and Chakwera should qualify for mental examination' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'MCP says Malawians best judges on who between Mutharika and Chakwera should qualify for mental examination' to a friend
Lilongwe Msozi South MP Vitus Dzoole Mwale told Parliament that president of Malawi Congress Party (MCP) Lazarus Chakwera,has rapidly gained ground...
Being mentally ill is when 1 at the age of 79 says is young while considering others to retire at the age of 65 for being old
Wathuyo Pitala ali bwino-bwino. Koma uyo Lazaloyo ndi amene akufunika ku Mental. Nzosatheka kuti Pitala angadwale misala asanayambe Lizaloyo. Ayambe wakatcheketsa kaye Lazaloyo kenaka mubwere mudzamutenge wathuyi. Pitala wanenetsa kuti dziko likuyenda bwino magetsi akuyaka bwino bwino, Anthu akefe olo kuba olo. Akumaba kwambiri ndi Atumbuka nchifukwa chake bwana anati mmipandomu ngati ku ESCOM ndi MACRA ndi enable otelowo tiikeko Achilomwe pang’ono kuti kubaku kuthe. Simwaona zasintha?
MCP ndi DPP zipani ziwirizi zonsezi palibepo chazeru zimene akuchita apa zikuwoneseratu kuti si azisogoleri ayi osewa kutukwana akutukwanaku Sichina koma kufunisisa kuti azikaba palibepo msogoleri apa mulungu atipasira musogoleri woti athandize zikoli amalawi izi sizitithandiza ayi tipephere kuti mulungu alowelere.
They are all mad, they know each other!
You can just look at the faces and know who is lying/Who needs psychiatric attention. Even kalankhulidwe will show you who is mentally challenged. If you need me to spell it out for you then its BWAMPINI
People are talking as if it is only DPP or the President who has seen mucous in Chakwera’s speech. Where do you put the Speaker’s order of not including abusa’s insane speech in the hansard?
Chakwera, the dirty new broom which is failing to sweep smartly, desperate to rule, he has resorted to develish and unchristian language, man of collar, slow down. The more you use angry and abusive language the more Malawians are realising that you want power due to bitterness and not necessarily to help Malawi. Hang with your bitterness while Malawi seeks solutions to its problems. After all there is nothing you have said you will bring other than american accent. Your nonsense MUST STOP.
Ngati chakwera walakwitsa apresident kubweza ndi kunyoza. Kodi apart from kune ”incopetent, ineficient” kodi a achakwera akunana za kubazo? ndiyankheni chonde abale
DPP are thieves and the president himself is the prince of thieves as said by the genius Chakwera. This pathological liar is taking us to great sufferings.
The whole MCP leadership is mentally challenged, including its followers. Making blunders out of hate and njala yofuna kulamulira dzikoli. Wait for 2019 when you will know the truth.
A Malawi tatopa ndi ndale zotukwanizana – ana anu akuphinzirapo chani apa?
Tell tht to MBC u brainwashed…
peter is mad