Email a copy of 'MCP south chairmen back Chakwera ahead of Chikwawa rally: Dzombe, Jumbe are ‘confusionists’' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'MCP south chairmen back Chakwera ahead of Chikwawa rally: Dzombe, Jumbe are ‘confusionists’' to a friend
Malawi’s opposition People’s Party (PP) continues to sail through existential crisis and has stopped Khumbo Kachali’s intentions to start conducting political party...
zikomo kwambi a malawi kuti mwadziwa choonadi ndipochoonadicho chidzakumasulani mu 2019.
I don’t support but neutral but I can see that MCP is the strongest party not these coming breifcase parties.
Malawians let’s be crefull these new parties are there for their personal gains. A political party owned by a family ???????????
Anzathu a gule wamkulu musamalimbane ndi mark my words. There is no word worth marking here. Reality on the ground is that MCP kumwera muiwale. May be after several generations not until Nanga bwanji maflopa pa ma recent bye-elections. Inube mudzalira mpaka kale kumanamizira kuti mwabeledwa chisankho. Bola UDF kapena mai uyu wa cashgate akhoza kupezako timavoti kumwera koma osati MCP ayi. Uku ndi kwawo kwa Mapwiya basi. Anzanu agule mamkulu ndi anganya ena tinkawauza tisanavote in the last elections koma makani awo ngati othena agaru. lero ali nyonyopilili kuvomereza zomwe tinkawauza. MCP Kwachaaa kwachaaa. Kwacha lero? Kumwera kudacha kale… Read more »
khalamba zokhazokha even Peter munthalika khalamba.Malawi kuvetsa chisoni
If we want a better change, MCP is the best option. DPP, PP OR UDF have failed the nation. Mark my words.
Pano chipani ndi Mcp.Ndiwozungulira mutu yekha amene akuyang’ana za Dpp.Dpp has totally failed Malawians in everything.We can’t wait to have Chakwera as our president.
Anthu Ena Mukuti Mcp A Mcp Ok Simudawone Zimene Tinaona Ife Try It ndi Njoka Zaanthu,if He is one of Cashgate benefiiacers Nanga Azalowa mboma azaba bwanji?
Dont live the old thoughts. MCP is the best party to take Malawi to the best levels
Mtunda udakali. Only short sighted and those who don’t follow history think the economy will be like this ntil 2019. U work on the present and think ur there. But ur friends are working on the future. MCP work up!!! U will cry the same way u did In 2014. Just a tip, In 2004-2005 Dr B Muluzi gave Bingu no chance for the 2009 Elections because of the ame issue, Economy. Later in three years time the economy picked up overshadowing the hardships in previous two years. He was the popular presidential candidate. Zisankho mwachita za pa region kaya… Read more »
Koma Jumbe walingalira bwanji Dala,osaphuzila kwa anzako achina Sosten Gwengwe,Abel Kayembe,iwe bwinotu dziko lozungulira ili..
A Drogba ndi a Mapwesela mukayang’ane nkhope ya a Pitala Mathanyula,a george kaziphwisi chaponda ndi a badall gondwe ndipo muzayamika kuti anthu mukuwaona pa zithunziwa ndiooneka bwino nkhope zawo olo mwana wanga akamalila ndikangoti, tonthola ukapanda kutonthola akutenga ndipo nthawi yomweyo mwana amatontholelatu.