Email a copy of 'MCP’s Chidaya laid to rest: Chakwera gives powerful eulogy' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'MCP’s Chidaya laid to rest: Chakwera gives powerful eulogy' to a friend
Politician-cum-businessman Iqbal Omar has unleashed a withering attack on the Malawian President Peter Mutharika accusing him of mismanagement of the...
Was a man indeed, a man with principles. Let us not forget what we learn from these people
MHSRIP.
Bambo Chidaya bambo anga muuse mumtendere. God be with you all the time. R.I.P
May his soul rest in eternal peace.
Ndidali pomwepo mmene anthu adali kulankhula molira. Ifa ya Chidaya itiphuzitse a Malawi tonse khalidwe labwino, lokonda upemphera, lokonda dziko lathu, lokonda Chipani chathu, lokonda umodzi. Kulankhula kwa Gondwe mmalo mwa zipani zotsutsa kudandigwira mtima kwambiri maka maka pamene adzakambapo za mikangano imene ilipo Mchipani cha MCP chimene anthu akuchiyembiekezera kupanga Boma mchaka cha 2019. Mamembara a Chipani amene mwagalukira mtsogoleri wa bwino, wowopa Mulungu, nzeru zanu zili kuti? Kodi mufunadi kuti mchaka cha 2019 MCP ilamulire dziko lino, kodi maphokoso amamanga mudzi, dziko kapena Chipani? Msatero ayi. Imfa ya Chidaya ikhale yotiluzamitsa tonse ndi mtima umodzi kuti motsogozedwa ndi… Read more »
May his soul rest in peace
He was gentle man served for all four president of MCP Ngwazi Dr Banda, Gwanda Chakuamba, John Zenus Ungapange Tembo and incumbent Prof Lazarus Chakwera. Rest in Peace Portipher Chidaya.
I will remember Potiphar Chidaya for the revelations on JZU. May his soul rest in peace.
may you rest in peace bwana. mwatisiya mmavuto mwa agalatiya osunga ndalama mmanyumba, mma car boot, mma pilokesi, mma account a kunja olo mmaina aazibale awo, milandu yake yosakambidwa olo kufufzidwa. aahhh tuweta njoka mm massion bwana. tikupempherera mzimu wanu bwana. tikukulilani, tazivera tokha- kudziwa komwe ndalama yacokera koma ndi yanji. enawa ndi envelope phatiphati
cisazo cabwino bwana.munatiphuzisa nchito ndipo ife amene timatsata zincito zanu ndithu sitimakhala ndi nkhawa. koma cimwemwe mu ntima. ZIKOMO BWANA NTIMA OKONDA KULANGIZA