Email a copy of 'MCP’s Kondi Msungama face theft charges: UTM’s Saonda an accomplice' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

19 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
Nambewe Sokosi
Nambewe Sokosi
5 years ago

Why are you failing to arrest mbava zinzanu zaku DPP ko, yet you find it so easy to arrest those in opposition? vuto nchani?

mjiba
mjiba
5 years ago

Mbava zokhazokha. Chimene chikudabwisa ndi chokuti nkhani ngati imeneyi chifukwa chiyani ili ku Lunzu second grade magistrate court? Bwanji osakalowa nayo ku Blantyre First Grade magistrate court? Kodi mukuyang’ana zilango zimene angapeleke second grade pofuna kuthawa kukhwizidwa moyenela? Nkhaniyi inachitika malo ambiiri kuphatikizilapo pa immigration yomwe ili mutauni, ndi chifukwa ninji mwapita nayo ku lunzu???? Chonde a Director of Public Prosecutions lowerenipo apa pasanaole, awa ndi amene akumadyela ma Burundi kumagulisa citizenship. Akwizingeni

DAVIE C MAKAWA
5 years ago

i dont see the truth in this story, if this was true you would see the mutharika broadcasting corporation taking it to some level because thats what they are bussy searching for, at the moment.and there is no way UTM and MCP can break a deal together.

123
123
5 years ago

This is definately Tit for Tat where were you all this while? Why are you targeting member of opposition at this hour? When the Elections are around the corner?Something is not adding up here, everybody knows that DPP government is corrupt to the borne. Let the opposition do their campagne freely, without intimidation or fear, and bring them to book after the elections is over. If your motive is good.

Kennedy
Kennedy
5 years ago
Reply to  123

Do we suspend laws due to pending election?

bullets
bullets
5 years ago

Wa MCP uyo khalidwe lake nde ndi imeneyo. Kukhalira kubera anthu. Analipotu anzanu ankachita zomwezi koma lero anapita osatsazika.

Mvuu
Mvuu
5 years ago

Writer, atleast u would have indicated a date wen the office was committed otherwise in this period of campaign such accusations will be regarded as a weapon by the gorvernment to silence the opposition, totally killing democracy

Jesuit
Jesuit
5 years ago

Kuba nkwa magazi awa. Shame.

Mulomwe
Mulomwe
5 years ago

MCP aspiring MP Msungama is such a crook. Nde azalamule awa? Mbava iyi Msungama has always been a crook… I remember this guy Msungama in Chinyonga from the 90s… crook oyipa uyu! Nde azakhale MP azatibera koopsa

ndele
ndele
5 years ago

olakwa azingocelatu sitikufuna anthu abisalilekoku zipanizi ai.vutola kusadziwa kusiyana kwa kuphuzila ndikuzindikila.

China
China
5 years ago

Ndunama ndiokuba uyu kuyambila kale

Read previous post:
CCJP’s debate initiative excite female contestants

Female contestants for the May 21 2019 tripartite elections in Mangochi District have commended the Catholic Commission for Justice and...

Close