Email a copy of 'MCP’s Mlomo now UTM regional governor centre ' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'MCP’s Mlomo now UTM regional governor centre ' to a friend
Nyasa Big Bullets' Confederation of African Football (CAF) Champions League opponents, Gor Mahia of Kenya were in England for training...
You UTM guys be careful who rides ur band wagon of transformation. It is indeed a right of association but some of the guys u are welcoming need to be in the back seat not on the steering. This guy has nothing to offer. Track him down to the constituency he once presented u will see that he is just a spent material. Watch out who u mingle with, u will de-campaign urself.
A Mlomo,
Choti mudziwe ndichoti a UTM sakufuna madala ayi, inuyo ndinu mdala, mukungofanafana ndi PETER. ngati pamsonkhano waku Salima munalipo, panali mafunso oti. kodi nkhalamba imathamanga, imayimilira, ima khala ndi mphamvu? anthu anati ayi iiiiiiii! ndiye inuyo muthamanga?
Akuti barely weeks after utm blah blah . Lol
If you understand financial markets you know that a party has more value at launch then the value wanes over time.
Any rallies chilima holds will simply seek to reduce the waning but won’t upp utm odds
Mcp siyikugwedezeka inu nkumati muli ndi governor meaning mlomo,,,,kkkkk….achinyamata munkafuna kulibeko Ku utm?Mcp yidazitaya kuti zidatha ntchito
This is where MCP is going to loose. You have purged off all the old guard in every district in the central region , I don’t know what strategy that is. A person has either to be a Chakwera bootlicker or wa Assemblies of God. A Chakwera akazawina , Kamuzu azadzuka kumanda.
To me Dr Chakwera downstairs really care about leading the country, he has no policies nor strategies, as long as akulandira ndalama za u leader of opposition and kick backs from the likes of Khatio, he is ok
Nsanje….Chakwera ndiyo ise tasankha. Wanu was Catholic… Kaliati..Catholic.. Masangwi..catholic…Kalindo. Catholic….Malunga catholic…..we voted skc walephera we want others….calister Catholic
some pipo u pick or join us Will destroy and demotivate us. This old man is not liked by pipo
Chipani kusowa Anthu mpaka kumapita kunkhuti Kwa MCP kumakatola zowola za ntchentche. This is a party of scavengers kudya zowola ngati khwangwala. Kenako mukatenge Foloma Mwale ndi Bester Majoni. Mukatengeso Felix Jumbe akuwola ku dpp.
ma cadet mulibe nfundo kwanu nkulila basi mutate ndinu,
Anyamata a UTM akundisangalatsa achoka ku DPP kuti Peter ndi wamkulu kwambiri sangathe kuyendetsa chipani and here there are parading another old fellow as their central region strongman. When have you realised that you need old people as well? What is it that you have seen in this old man? Yet you were daily bad mouthing Peter Mutharika that he is too old to run the affairs of the party and country? So Agogo anu ali apawa a Chilima alimba 2019 popeza inu mumafuna achinyamata othamanga magazi okhaokha kapena mwaiwala chifukwa chenicheni munachokera ku DPP.
Mbava izi
Mlomo was a useless politocian to both MCP and the whole nation. Akagweretu ameneyu. He can he can go to the losers team. Kafucheche ameneyu. Nkhalamba yachabechabe.