Email a copy of 'Minister Massi says diesel generators to arrive in Malawi ‘soon’' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

1 Comment
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
LIPHAVA NAMANDWA NGONGOLIWA
LIPHAVA NAMANDWA NGONGOLIWA
6 years ago

Ife a DDP ndi anyamata anthu ku Escom tikuyisasantha tikuyimeza tikuyikuzula tayibela…kuyivinitsa bungwe limeneli. Atsogoleri akale samaba mokwanira ngati ife. Ankadziwa ndani kuti ikhala pamaondo? Mumayenda mbali Amalawi. Mablackout wa mungowazolowera basi. Muzizikanda mumdima ambwiye. Ndinthawi yathu ino olamulira.
Magenset wa ndi tikungokutsukani pa kama kuti tiimalize Escom yi kuibela bwino-bwino. Tiikombeza. Ife zokonza magetsi wa chidwi tilibe ataaa!!!. Ife tizingugula ma genset ambiri basi osatinso kuika makina pa mitsinje kapena ndi dzuwa. Aiiii!!. Zopusa zimenezo muzangodikila a Congress kapena a Chipani cha Amai olo Chafuko 2050 tonse titalowa kaye mmanda ndi adzukulu athu onse.

Read previous post:
TNM Mpamba pumps K6m into St John’s Hospital in Mzuzu

TNM Plc, through its mobile money business, Mpamba Trust is proud to announce a contribution of medical equipment worthK6 million to...

Close