Email a copy of 'More at risk of preventable deaths: Malawi hospitals facing services scale-down' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

33 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
Please
Please
8 years ago

Kodi a Kapito alipo Ku Malawi?

bad
bad
8 years ago

Which DHO can call a nurse like you. A shadow minister amenewo. Badikirani…………Sonkherananitu ma allowance aja mwadya 9 weeks. That’s what happens with Cash Budget. The whole shadow minister does not know this………………….Shame………Just tell the Malawi nation the truth not politicking

nowa titsekulireko
nowa titsekulireko
8 years ago

tikhonza kuyankhula izi ndi izo koma tonse tikutha psyiti. Sizinafike pakolasi,zipani zilamulira zambiri palibe chitazasinthe,watch out yesu akubwela posachedwa.

Foxyandy
Foxyandy
8 years ago

Tidapita pa chipatala chodziwika cha m’boma la Zomba.Adalemba bwino lomwe mankwala amphumu(sulbutamol), adatipatsa bactrim ndi asprin. Titawafunsa akuluakulu,adangotenga mankwala oyenera nkutipatsa.Akumidzife tili pavuto lalikulu, TIKUFA!

Decent Citizen
Decent Citizen
8 years ago

Pitala ndi alomwe anzake asiye kuba and the rest will follow suit in Malawi.Ngati kuba kumayamba ndi anthu akuluakulu with all the benefits under their feet,what do you expect from an ordinary struggling worker?Its has become a norm in the civil service to steal to make ends meet.

Aron
Aron
8 years ago

Peter mwalephera boma tangochokaniponi pampandopo

Dambudzo Mwasanya
Dambudzo Mwasanya
8 years ago

The Health sector in Malawi is crap.Very few doctors to carter for the bulging population.Some crooked pharmacists sell drugs to private hospitals.No proper funding to hospitals since everybody in higher positions is concerned with self enrichment.Poor diet for patients.Hospitals are killing grounds in Malawi.Nothing is working in this impoverished country.Lunguzi pump some senses into these dunderheads.They don’t seem to have any idea on health sector.They are politicising everything.

Mwamuwunda
Mwamuwunda
8 years ago

But closely monitor the so called health worker not to be stealing drugs yet the hospitals are struggling.

Karonga citizen
Karonga citizen
8 years ago

Kunonso ku Karonga a chipatala afika pena pake poti ay, zosayenda. Kukhalira kupemphesa koma ili ofesi ya boma. A Malawi, kuba tisiye. A ndale musiyenso dyera kuti ndarama zizipezeka. Anthu opeza bwino azilipiranso.

gongonyeke fupa la nyi..

Iwe N0:21 ngati umadya nowo mamphemvupevu khala chete ndizokhudza amphawife izi osoti agulukunyinda ngati inu ndi mbava zopanda chisoni zinzakozo.

Read previous post:
Kaliati mobilizes Malawi women to form professional networks

The Ministry of Gender, Children, Disability and Social Welfare is mobilizing women in Civil Service Commission to form professional networks...

Close