Email a copy of 'MP Chakwantha ‘hands himself in’: Malawi WhatsApp coup plot' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'MP Chakwantha ‘hands himself in’: Malawi WhatsApp coup plot' to a friend
Former students of Bwaila secondary school will Sunday, 27th February, meet at their old school campus in Lilongwe where they ...
Pezani ma advisor anzelu osati mbavazo zikuyipittsilani mbili enawo ngakhale kunyumba kwawo kulibe mtendere. Pezani anthu akuthandizani kukoza zinthu. Sukulu imachotsa umbuli okha koma uchitsilu suchoka
okondedwa nonse a Malawi anzanga tiyeni ifeyo tisamakolezelenso moto zinthu zachonchi zikamachitika mudziko mwanthu muno,kodi tonse pamodzi sitingangogwa kuti Mulungu atikhululukile machimo athuwa?coz izi zikuchitika bcz of machimo omwe adzadza dziko lino
apitara ndiye mukkunamizidwa manga angati,bushiri akuthandiza anthu inu mukuti akufuna mpando wanu, mpandowo siwanu ayi panali kamuzu ,bakili,akulu anu,amai,so who are u to intimidate us nthawi ya reflandam munaliko inu? mukukolola posatulusira thukuta.36/ percent ndikuluza kumeneko.cardiirc is ffollowing
Achoke pampando tikukamba ndife a Malawi. Don’t bullshit us you are childish. Simungalimbane ndi MCP munya muona agalu inu. Landslide yachani ngati zikukanikani pano. Anthu sakufuna.
Hahahaha . U can’t fight the government.
Wayiwelenga ameneyu kkkkkk. Akuziwa kuti akagwidwa masana akagona konko. Kutentha kumeneku kumakagona ku cell eish!!! But he is not a hero coz he has done nothing for him to be called a hero
Only the courts can prove someone innocent or guilty.
Peter ndi mbuzi yopanda mano mkamwa chitsiru cha zitsiru zonse muno mu Africa
Peter Chitsiru cha president, Peter ndiwe mbuzi I have never seen a silly president who is also clueless and brainless. Thats why nvula yakuvutani ku south agalu inu. munya muona agalu.
Well done boy, osawaopa awa. Am on my way in solidarity. Kwacha!