Email a copy of 'MP Harry Mkandawire claims $230 000 loot in Malawi embassies' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'MP Harry Mkandawire claims $230 000 loot in Malawi embassies' to a friend
Khato Civils is a black-owned African values driven design and construction company committed to contributing towards infrastructure development in the...
Thiefty is the slogan of DPP. Follow, follow, follow the leader. If you are DPP do what DPP is doing; “if you are in Rome do what the Romans do”.
So bwana Harry ndi auditor yemwe analemba nchito yowunika China muma embassy. Pitilizani nchito imeneyi. Takunyadirani.
Mphongo zogona kukhomokosatseka
The issue of passport not yet concluded.. ndiye pano tikumva izi.. takatani anyamata ndi madona, azibambo ndi azimayi.. ndi nthawi yanu.. nanga nkutani ngat akulu akulu akugona… or ali pa sogolo ndi zichitochito ngat zomwezo
DPP inatumiza alomwe okhaokha ku ma embassy, kuba ndi khalidwe lawo
Dude are you for real? Monga zooti mma embassy mwadzadza a Tumbuka si ukudziwa? Koma iwe umadzitsata bwinobwino? Mwachitsanzo kuno ku South Africa bwera uzaone. Tisiyeni alhomwefe tipume please.
Harry Mkandawire, a northerner, should be worried about MCP who claim that the North does not deserve the level of development it is getting under DPP. The MCP spokesperson on financial matters told parliament on Monday, 19th February that the North was getting too much development compared to other regions, despite the north being the least populated region. This means that in the very unlikely event that MCP wins elections next year, development in the north will grind to a halt. Therefore, vote wisely northerners.
Zamkutu!