Email a copy of 'Mphwiyo hospitalised, Kauwa released on bail' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Mphwiyo hospitalised, Kauwa released on bail' to a friend
The ruling Democratic Progressive Party (DPP) has rejected claims by Peoples Party (PP) that chief Cashgate suspect Oswald Lutepo is...
mphwiyooooooooo ! Dzina ndi khope plus khalidwe ndende kufafana
ndine mbuli pa nkhaniyi.
kodi nkhani ya Bakili ija bwanji? yoba ndalama za boma ija? imamugwetsa ma disc ija?
Mphwiyo ku court ananena kuti iye samaba he is hardworking young man mpake ali ndi mansion ija, ndi ma benz ndi ma fortuner ngakhale salary yake ili k250,000. MRA inadabwa pamene paja kuti chuma chonsechi muli nacho bwanji simukuonesa ma record opereka msonkho? Anazipachika yekha ameneyi. Plus ndalama ya bail K15 million anatulutsa mchikwama ameneyi, amfufuzenso account yomwe zinachokela.
Akulu akulu lest be honest,this MRa guys are being unfair,Mr Karim Abdul Karil Batatawala of Lido Electrical has been charged 17 billion for tax invasion in 2012 but the story is still on because Batatawala is busy corrupting government official and MRA staff to have his case cancelled.I salute one Mr Ngutwa who was the Director of Investing @ MRA for being 2 professional on how he handled Batatawalas case but to our surprise Abdul Karim Batatawala dished out millionz to one top offiers @ MRA to oust Ngutwa and ngutwas contract has been terminated.Malawianz read this with interest and… Read more »
Hell is on earth Bruv.You were a hero by then when you were swimming in illgotten riches and now time has come to reap what you sowed with the crooked old Mum who praised you that you were a no nonsense budget director while deep down you were swindling billions meant for the impoverished Malawians.You have forgotten the money you were splashing at Golden Peacock like you won a lottery.A mere civil servant who was living a Hollywood style.These people are not heroes but mere thieves.Some of us are not concerned with these cooked up illness.You lock up people with… Read more »
Zayamba kukuthimba tsopano. Kumangolongeza chuma cha boma m’thupi umati mtima usatupe? Ayi chirani kuti muzayankhe machimo anu pansi pompano
Never thought mphwiyo has a heart, if he has one he could not have put millions of people now suffering in malawi through his actions. Please please kick him out of hospital
MW pcells&prison are graveyards he’s not fit for it anapangidwa operation yovuta muthuyu
koma yes zimakoma ponjoya ena kumaoneka useless ngati sanapindule ndi mkalasi osadziwa kuti mukuphatikiza ndi kuba zonse. shame