Email a copy of 'MPs want K4bn Constituency Development Funds by December' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'MPs want K4bn Constituency Development Funds by December' to a friend
Audit General’s Office has observed that the current Integrated Financial Management Information Systems (IFMIS)- a technical solution to deter corruption in...
Chakwera, CSOs and the media should apologise to president Mutharika for criticising the K4 billion fund when actually MPs and their constituents need the money.
Anduna, musawapatse mpaka Chakwera ndi azinzake ngati Mtambo, Trapence Kajoloweka ndi ma dunderheads ena omwe ndawaiwala ayendenso kukapepetsa kwa APM ndiponso Chakwerayo ndi azinzakewo avomereze kuti zomwe anachita zija zinali za ulukhu.
Aphungu enawa sabwelera Ku nyumba ya malamulo angofuna kuba ndalamazo. Zitsungeni ndalamazo, mudzawapatsa aphungu omwe apambane pachisankho cha 2019.
CSOs agwa nayo. You demonstrated against this money, lero opposition MPs are crying for it.
Opposition MPs now want the K4 billion. Didn’t their confused leader, Chakwera march against the money?
MPs think Malawians are mabulutu. The MK20 million wasn’t meant for any constituency development at all. This money is meant for their pockets as a token of appreciation……they know it and we all know it. In any case what type of projects can you do with MK20 million. MPs are not in parliament for its people but rather for their pockets. Remind me again why MPs get paid??????
Kkkkkkk. Tsono opposition you now agree that mwagwa nayo? Inu simukadziwa kuti ma big a Goodal ndi mdambo modzimira moto? Tsono ma CSO ndi Chakwera ndi a PAC muwauza chani pa ma ultimatum awo aja? KKKKKKK. Bola Chilima wangochita cut and paste movement ya ku Zambia NAREP nkuibweretsa kuno.
Ine waku Ekwendeni olo a MP nyamuyaba muwapaste CDF sangawine.
You want to cheat us that you will accomplish in three months what you failed to do in five years??? Idiots! Munya muwona!