Email a copy of 'MRA assists flood victims with 2 million Malawi Kwacha' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'MRA assists flood victims with 2 million Malawi Kwacha' to a friend
The Malawi Revenue Authority (MRA) says it will join the World Customs Organisation (WCO) in the commemoration of the 2015...
Kodi mukuti staff ya MRA ndiyomwe yapanga donate kodi ndalamazo atatolera anakaziika ku account ya MRA. Check the cheque mukufuna kunamiza ndani kodi. Or is it a Social Welfare Account ya MRA. Muzinamiza osapita ku school zimenezi.
Koma a Malawi especially those commenting on Nyasatimes ndinu omvetsa chisoni ndi umbuli. Your literacy levels are so low. No wonder most of you here failed simple MSCE exams. Read and understand the story first before commenting rubbish. MRA as an organisation doesn’t give donations. It’s MRA staff who contributed each a minimum of K500 to reach that amount. Inu amene mukuti yachepa yanu ndi chani ntchito kumwa ma sachet basi.
Was the money donated in the name of MRA as an institution or from staff members? Because the heading and the content of the story do not correspond positively,the heading says MRA has donated and the content says staff members did because if members of the staff did generate the funds then it shouldn’t be said that MRA donated rather it would be MRA staff have donated otherwise MRA is not authorised to donate any single tambala to any organization under any circumstances they are only authorised to collect taxes not to spend them in any way or the other.
koma zoona mra manyazi mulibe awa ndiye maliro ka two basi ndikaigawa ndi omwalira 200 inu amaratio mukupezano bwanji, mbava zobera likuswa mtengo
This must be the worst joke i have ever heard. MWK2 MILLION FROM MRA …The only tax collecting in the country, which just recently reported a 229 billion collect in 2 quarter..Comr on…MRA is not a profi organisation.It saddens me that we have a selfish goverment like this..its Hogwash!
zomvetsa chisoni kuti abale anthu apita moteromo, mizimu yawo iwuse muthendere.
Lady in red, ahhh, ukufana ndi nkazi wanga wakele kukongola, wanva?
Why two million only.shame mra
Generated wachani apa,ndalama za misonkho mwayambapo kuzigawa ngati zanu?Musayambepotu apa,mumapanga bizinesi inu kuti mukakhale ndi ndalama zogawila anthu inu?
Come on friends, understand english.This money did not come from MRA as a body but from staff working at MRA.Did i miss something here?