Email a copy of 'Msungama resigns as Bullets chair: Supporters broke into club offices' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Msungama resigns as Bullets chair: Supporters broke into club offices' to a friend
Unknown criminals on Friday shot and killed one of police detective officers who foiled a robbery in Limbe, Blantyre. Southern Region police...
Kkkk koma BIbi chimidzi heavy
Kkkkkk kugenda kuja unkango zitengera wekha mavuto neba kkk
Neba yako yija sudzathekaso basi ife ndiye zisatikhudze!
Kondi u ll regreat this…..watinyazisa hevy…….ngongole zako umaziputazo upeleka wekha…….sure stream ndilandile……
Inu Dan munkati za ndalama zingayende. BB iyendetsedwe bwino tsano
Takuonani munabwela ndi mtima wofuna kupha team yafukoyi musazabwereso
kwatsala Harold Fote, ameneyu kunyenga azimayi ndi matama too much. Anamchotsa ntchito coz of matama and no performance ndi kunyenga mzimayi amene abwana ake ankamutsilila. Ku TZ ananyenga hule plain kuthawa kulipila this is the worst bullets I have seen as a Trustee.- koma bury everythn focus on the game this Saturday- Red Army woyeeeee!!!!
Ndiye mukhanilanji kuti ndinu a BULLETS amene munayambitsaa zipolowe pakat pa Silver ndi Mighty. You BB supporters are vandals, crooks Villains, robbers,thugs, you name it. This team is just a group of disorganized thieves
It’s sad that Dan has decided to take advantage of the situation and steal 2 Million kwacha. It’s the same Dan who brought a musician from outside Malawi and failed to pay her/him mpakana munthu kumapemphesa transport yokuti azibwelera kwao. Where do u get people like him to run the affairs of a struggling entity like Bog Bullets? U have brought shame on our beloved team. Entering CAF was a big mistake. Anyone with the right senses knew this was going to cost bullets a lot. Now they have stollen all the money that had been raised and they have… Read more »
Kuzibera mnyumba mwako mom we,koma BB.