Now this is social media. Nothing stops us from discussing this issue. Mulli umbavha wachuruka. Kodi mose muja munayambila kumba ndalama zaboma simuna khutile? Kodi ndalama zomwe munaba through National Bus Company which you ran underground simunakhutilebe? You are very evil you should be shameful of yourself stealing in broad daylight ngati imeneyo. Gagging UTM et al is not going to work. You are simply trying to raid government funds and Malawians are watching you.
Nandolo
5 years ago
Eight more months. Pang’ono, pang’ono, pang’ono!!!!
Nduzayani
5 years ago
Mulli tsiku lako lizakwana uzasiya cz ukusewera ndi ndalama za anthu osauka ku Malawi.Kutenga chiletso kuti uziba?Kuli Mulungu kunjaku nyanga ukusambazo zizatha ndithu
nafeso amalawi moti tilimbane ndi boma popeleka madandaulo athu tikulimbana ndi chuma cha anzanthu. The laws of this country allows someone to claim from government to pay for damages caused by fellow citizens using tax money. remember he has the right. next time let us avoid attacking personal property when demonstating otherwise I see more money being paid ife tikaononga
Nzika ya Malawi
5 years ago
Mtima suukhutadi ndithu! A Mulli chuma chonsechi koma osakwanitsidwa ngati mudzapita nacho kumanda? Kuba misonkho yathu momwemo! Mulungu akulangeni ndithu! Mzipatala mukusowa mankhwala koma kumangoba munthu wopanda mzimu iwe! Ngakhale upange gag UTM ife sitisiya kuyankhula. Mudwala nacho chokolo!
Ntengo wa Kesia
5 years ago
Most of us saw this coming: Mr Mulli has every right to claim for the damages, including intrinsic damages, arising from the savage demonstrations.
And he also has cause for getting legal restraint against UTM (the Bus Company) officials, and even Kajoloweka. That is how the Law works in a democracy.
Asa.
Nalingula
5 years ago
Tiyeni Nazoni ndinu Ana Kamozi.Vuto ndi Amalawi sachedwa kuyiwala ….Chasowa ,Njaunju RIP.Kupanda the Palm Wine Drinkered kukanizidwa Udindo bwenzi mukadali chete koko.
Reginald
5 years ago
Can your father match Mulli ?
MA D7 MA D6
5 years ago
VUTO LOSAMBA VINYANGA MMALO MODALIRA CHAUTA !!!
nyoko
5 years ago
In Malawi, those who prosper are always suspected as long as he/she is a native.If you are Chines or Indian No problems. This spirit is in all Malawian despite whatever status he is. Surely ,Chilima and Jolokamo support Mob death ,attacks and destruction of both property and lives of people.If business is all about conducive environment why should these knowledgeable citizen be against the step the fellow citizen takes to protect and teach this government about its responsibilty. Parliament has been very quiet on Mob. People are still loosing lives property , Mulli Teach these Politicians to stop Making nonsense… Read more »
Apumbwa
5 years ago
You an gag them, but we wont stop talking, Malawians will continue to talk about you and Mr Maliseche, Freedom of speech is our God given right
Now this is social media. Nothing stops us from discussing this issue. Mulli umbavha wachuruka. Kodi mose muja munayambila kumba ndalama zaboma simuna khutile? Kodi ndalama zomwe munaba through National Bus Company which you ran underground simunakhutilebe? You are very evil you should be shameful of yourself stealing in broad daylight ngati imeneyo. Gagging UTM et al is not going to work. You are simply trying to raid government funds and Malawians are watching you.
Eight more months. Pang’ono, pang’ono, pang’ono!!!!
Mulli tsiku lako lizakwana uzasiya cz ukusewera ndi ndalama za anthu osauka ku Malawi.Kutenga chiletso kuti uziba?Kuli Mulungu kunjaku nyanga ukusambazo zizatha ndithu
nafeso amalawi moti tilimbane ndi boma popeleka madandaulo athu tikulimbana ndi chuma cha anzanthu. The laws of this country allows someone to claim from government to pay for damages caused by fellow citizens using tax money. remember he has the right. next time let us avoid attacking personal property when demonstating otherwise I see more money being paid ife tikaononga
Mtima suukhutadi ndithu! A Mulli chuma chonsechi koma osakwanitsidwa ngati mudzapita nacho kumanda? Kuba misonkho yathu momwemo! Mulungu akulangeni ndithu! Mzipatala mukusowa mankhwala koma kumangoba munthu wopanda mzimu iwe! Ngakhale upange gag UTM ife sitisiya kuyankhula. Mudwala nacho chokolo!
Most of us saw this coming: Mr Mulli has every right to claim for the damages, including intrinsic damages, arising from the savage demonstrations.
And he also has cause for getting legal restraint against UTM (the Bus Company) officials, and even Kajoloweka. That is how the Law works in a democracy.
Asa.
Tiyeni Nazoni ndinu Ana Kamozi.Vuto ndi Amalawi sachedwa kuyiwala ….Chasowa ,Njaunju RIP.Kupanda the Palm Wine Drinkered kukanizidwa Udindo bwenzi mukadali chete koko.
Can your father match Mulli ?
VUTO LOSAMBA VINYANGA MMALO MODALIRA CHAUTA !!!
In Malawi, those who prosper are always suspected as long as he/she is a native.If you are Chines or Indian No problems. This spirit is in all Malawian despite whatever status he is. Surely ,Chilima and Jolokamo support Mob death ,attacks and destruction of both property and lives of people.If business is all about conducive environment why should these knowledgeable citizen be against the step the fellow citizen takes to protect and teach this government about its responsibilty. Parliament has been very quiet on Mob. People are still loosing lives property , Mulli Teach these Politicians to stop Making nonsense… Read more »
You an gag them, but we wont stop talking, Malawians will continue to talk about you and Mr Maliseche, Freedom of speech is our God given right