Email a copy of 'Muluzi case takes off, prosecution struggles: Some money erroneously added to K1.7bn' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Muluzi case takes off, prosecution struggles: Some money erroneously added to K1.7bn' to a friend
Malawians should expect somehow poor services from government as major revenue collector, the Malawi Revenue Authority (MRA) has last month...
Masiku omaliza sikudzakhala kulemekezana
Christopher,Ngwenyama,Imran Sadik,thank you guys for your comments!I have discovered that you have seen kuti a Chair is going to have a deep sleep soon!Nwo listen,once the government losess this case,then you know well we are going to make again a heavy campaign to resuscitate or kudzutsa boma lofaifa lija kuti a Malawi muyambenso kumakhala ndi makobili mmanja!Please agree or to disagree with me on this point!I salute you ku ma Court ko! watch Out, Muluzi is not old to rule Malawi again!
The case is clear, govt will not win this case because in a court winning is about having tangible evidence not hollowed evidence as given by the govt, but all in all God is living with all the truth and He is gonna reveal it on the last day!!
Atcheya Woyeeeeeee
Apa Boma tilipanga sue for wrongful arrest
Ka 10 billion kokha boma lilibe ndalama ili
Kkkkkkkkk
The case is already finished and Muluzi is a clear winner!
Just to follow the process angamati mulandu anaupondereza.
Its either the case was politically motivated or Muluzi is only being taken through the process of clearing his name by his DPP friends because he is a close friend to this illegitimate government. I suspect some papers of evidence that have been reported missing in this case were deliberately mishandled because for a case to be admitted at the high court there should be some preliminary evidence to satisfy the judge otherwise the judge throws away a case without a good evidence.
I strongly believe that the father and founder, Atate Ngawzi Kamuzu Banda( may his soul rest in eternal peace)was the only strongest one who new how to fight CORRUPTION.Though I was foung then, but when He saw that someone(worker)is living a life style above his income, he/she was being checked before it is too lae to determine where they were enriching themselves from. Malawians “Wake Up!” where are all these people who are building big mansions getting their money from.??? Was it not a fact that the Public Service was the least paid than the Private Sector??? But alas! look… Read more »
this world of ours !
Mukungogawana
Makobili apa
Wanthu wolemera inu
Wosaukafe kunangolira
Musiyeni Muluzi apume bwino anagwira ntchito
yopambana pa nthawi yake . A Malawi tiyeni tiphunzire kulemekeza munthu akanali moyo.
Pali zinthu zambiri zomwe tingapange zothandiza pa miyoyo ya anthu amene akuvutika mu njira zosiyanasiyana monga njala matenda ndi umphawi kusiyana ndi kumangoononga ndalama pa milandu
yomwe mukudziwa kuti boma silingawine. Mwaononga kale ndalama zambiri chiyambire mulandu umenewo and mukudziwa kuti boma silingawine bwanji osazisiya ?
Tiyeni tiwalemekeze atcheya ndipo potero tiwasungira moyo wautali kuti atiphunzitseko zinthu zina zomwe sitidziwa.