Email a copy of 'Muluzi presents Green Media Awards to Malawi environmental journalists' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

9 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
exvin
exvin
9 years ago

Mayo mayo ine !!!!! (crying) chilengedwe chikutha pamene ena akudyere momwemooo mayoooooooo!!!!!!!

Mowa
9 years ago

A waste of resources. What have they reported worth getting awards?????

Mwapheranjiru
Mwapheranjiru
9 years ago

Anthu amenewa amalemba ziani pamene chilengedwe chiri kutha! Zoona Rasta (No.1). Nkhalango, ndi nyama zamthengo zikutha atola nkhani osalembapo kanthu ai. Lero akulandira zikho za chani-amene agula zikho izi angofuna kuchuka basi pamene chilengedwe chikutha-za show biz basi.

Dr. Godfrey Mvuma
Dr. Godfrey Mvuma
9 years ago

While the gesture of awarding Environmental Journalists is a welcome idea, but Malawi needs to do more than just this in order to save this beautiful country. Malawi was beautifully Green during the process of developing the National Environment Action Plan (NEAP) in the early 90s. But now it is almost a desert. It is easily visible as you travel from Lilongwe to Blantyre. As a seasoned Environmentalist, I feel ashamed that we have failed the Malawian people.

chinkombaleza gumanyundo gowa
chinkombaleza gumanyundo gowa
9 years ago

Mukulimbikitsa kulemba nkhani mmalo molimbikitsa chitetezo cha nkhalango ndi a Polisi. ma gaurd a forestry nawo ndi ma WOOD GATE.; Palibe akuchitapo choteteza. Chinanso a boma mukukweza kwambiri magetsi mumati anthu aziphikira chiani. anthu akulephera ngakhale kuitanitsa magetsi chifukwa cha kukwera mtengo. Anthunso tanyanya kumangodula mitengo chisawawa ngati Mulungu namalenga sanakuuzeni kuti musamale chilengedwe. A boma mupite pa zalewa road block a police ndi aforestry akungogwira amene alephera kuwadisha. Chikhalilecho pantunda paja anthu akugulitsa akuwona osalanda. A muluzi chitani kanthu.

IIsshh
9 years ago

Comment number 2 by this Dr. seems misplaced. Not so?

Dr Isaac Chidyaonga
9 years ago

Let me start by thanking Nyasatimes for exposing this issue despite the fact that it is involving a high ranking official.
What baffles me is that Mcheka Chilenje is a very humble lady so I don’t understand why Mr Nkhoma wants to marry another wife.
But Kita was right to stop the issuance of the certificate becoz that was indeed against rules of natural justice.
God should forgive us indeed.

Mowa
9 years ago

What?????

Rasta
Rasta
9 years ago

Nkalango zikutha inu ndi kumalandila ma award achiyani. Kabwenzeni poti palibe chomwe mukuchita. Inunso ndi amene lkumagula makala heavy, koma nkhuni mwa Senzani. Ine nditakuzalitsani kaye mitengo kaye osati zachibwanazo.

Read previous post:
Kaliati in New York for ‘serious business ‘

Malawi's Minister of Gender, Children, Social Welfare and Disabilities, Patricia Kalaiti, MP, on Thursday held three separate engagements with NGOs...

Close