Email a copy of 'Mutharika ‘2019’ proclamations versus age, Saulos Chilima: Malawi Presidency' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Mutharika ‘2019’ proclamations versus age, Saulos Chilima: Malawi Presidency' to a friend
After being attacked at a rally by President Peter Mutharika and his frontline DPP troops for carrying a “bogus” survey,...
Tatopa ndi ulamuliro wa nkhalamba youths should take over
The warm heart of africa…
Another state funeral, another musolium
Don’t worry about 2919 just read what the Word of God says on Proverbs 27: 1. Then you will have your answer there.
Saulosi the writing is on the wall, please start strategizing 2019 is for the youth period.
Talking of 2019 now will only result to cardiac arrest to someone. I prophesy
Ine ndi dandaulepo apa abale anga a Malawi mwaiwala bwanji kuti Tate wa dzikoli Kamuzu Banda anatiphunzitsa Unity! kodi mukamati mtumbuka! mchewa ! muyawo mukulakwa mukuligawa dzikoli. chonde abale anga chepetsani zimenezi. tiyeni tionetse chikondi. Tonse ndife a Malawi. tiyeni tizikondana momwe a Kamuzu anatiphunzitsila. l love you all Malawians.
2019 is very far to talk of elections.build us a new stadium in Blantyre Mr president construct new roads and stop continuing where bingu left you must leave your own legacy
Kodi inu atumbuka , tulusani msogoleri wanu wokongolayo ndi wanzeruyo timuone . Nangaa kapena iju anali ” First Gentleman ” ndiye mumati ndi okongola, inu khope yosaona kuti yadyera ndiwo ya nkhwiru ija , kapena khalamba yanu mukuti Bima Shawa yi ndiye yokongola. Mukamalemba zinazi muzikhala serious . Ndikumasuleni , mtumbuka sazalamulira dziko lino kuzera pa mavoti, pokhapokha mutachita zija munamuchitira Bingu zi. Mzimu wawo uwuse mu mtendere
Atumbuka mpaka mulowa pansi chifukwa cha jealous. You will have your turn sometime in future. Do not loose hope. There is a better tomorrow to come. Peter is the worst leader sofar. How can he be talking of 2019 elections when he is failing to run the country now/ What a joke? Chakwera is ticking and ticking to the high office. It is now an open sencret. He is a better material for the top job and not Lomwe for its own sake. Where are the NGOs please/ When are we showing him that things have fallen apart?