Email a copy of 'Mutharika back from AU Summit on commercial flight: Says ADB pledge support for the youths' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Mutharika back from AU Summit on commercial flight: Says ADB pledge support for the youths' to a friend
Minister of Local Government and Rural Development Kondwani Nankhumwa appeared before the graft busting body, the Anti Corruption Bureau (ACB) investigators...
we need to be proud that youths will get something to do. Inu mukukayika zikayikani ife tikatenga ngongole zimenezo. Chilichonse chili ndi nthawi ndipo Mulungu salakwitsa, Enanu mufuna muzatenge ngongole atalowa chakwera? Kodi zamawa mukuziziwa? Mwayi wanzama ofukula ndi manja khasu lilipo wa achinyamata pliz let’s support Mutharika. Bible likuti iwe nyamata nyadira unyamata wako, ndiye mukudikira chakwera mu 2024 inu muzakhala Muli nyamata or madala?. pliz mwayi subwera kawiri, Ine ndi wachipani cha Nasfam koma ngongole ya boma ikundikhuza.
right hand yo nde ikuonekabe kukonyoka, linacika ncimake
tizazolowela zomwezi basi mmalo mokalima kumakagwadila anthu ngati awa, waste of time. so here again we go ADB —- komwe munakakongola ndalama zogulila cimanga ku zambia, mlandu on top mlandu wina, za pa my…lo
Ma negative reporter a paMalawi ovala silipasi. “Due to the ailing state of Malawi’s economy, Mutharika has been forced to utilise passenger planes” – umafuna akwere unpassengered aerial vehicle, kapena drone…kkkkkkkkkkkk
Sizachirendo izi. Bingunso antero koma ndalama zipangopita kwa macadet okha okha pomwe anyamata okonda zipani zina akungotuwa. This news does not bring any excitement to any God-fearing Malawian. I will rule the Gambia for 1 billion years.