Email a copy of 'Mutharika meets Malawi religious leaders: ‘Asks for special prayers’' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

22 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
shaaaa!
shaaaa!
8 years ago

Bingunso zinayamba chonchi.wa mwayi ndi mayi wa zingwe za mbuzi uja,chifukwa Chauta anamuonetseratu kuti sangalamulire Malawi.nde kumasamala zisanafike pa kadya kalista (cadiac arrest)pali chiphunzitso chachikulu kwambiri pamenepa.tiyeni nazoni. ali ndi khutu amve ndithu.

Abimu shawa
Abimu shawa
8 years ago

Akufuna kupempherela mvula or kudwala misala?koma inu palidi msogoleli apa bolatu JB.

Bamusi
Bamusi
8 years ago

Prayers for what? Mumangomtukwananso chauta INU. Kodi tinatonso ntikofiya kapena zisa za njiwa? Kuseli kwa phada kuli phwandodi.

me
me
8 years ago

The president have also of time to waste.

Mabattery a mlakho
8 years ago

Until now the so called professor doesn’t know meetings are just a waste of time.Kenako timva meeting ndi ogulitsa nkhumba,then oweta abakha…..akammanja….oitanira ma minibus…..ovina dusha……omenya madulira polowa mtauni……a zaufiti……list endless.A Malawi tili mmavuto.Bola nthawi ya John Chilembwe.Mayoooo!

benn
benn
8 years ago

Ngati Mtola khani anaulula za ma envolop kuli bwanji Mbusa kapena Pastor mukhala chete? Nanga womvera Mulungu pamenepa akhala ndani?

Kalithera
Kalithera
8 years ago

Kodi nanga aja a PP Livingstonia Quota System Church analipo, Ine sindinawawone , kapena sanabwere chifukwa anaitana si joyce Banda, ayi dikirani Joyce azabwereranso pampando, muzasangalalanso nayo Cashgate

ujeni
8 years ago

Kusowa zochita President. Very very clueless. Get a broom and go and sweep some dirty street we have plenty of them.

nanaphiri
nanaphiri
8 years ago

Alembi ndi Afalisi pose for a photo kkkkkkk moto kwa iwo opondeleza

Joseph Banda
Joseph Banda
8 years ago

No 5: Paja Judge Nyirenda amacokera ku Mulanje? Kodi mudzi wanj Bwana?

Ndiye ndinu opusa zedi

Read previous post:
Malawi campaign against fistula to restore women’s dignity

Minister of Health, Dr Jean Kalilani has said government with the help of UN agencies will prioritise the campaign to...

Close