Email a copy of 'Mutharika returns this weekend from New York' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

19 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
#DzukaniAmalawi
#DzukaniAmalawi
5 years ago

Whether he comes back over the weekend or next year in May just before the elections is neither here nor there. Malawian won’t miss him anyway. However, he will likely be voted in whether he is here or in the US. Says a lot about Malawian voters.

Bakha
Bakha
5 years ago

Koma ine ndilibe naye ntchito m’dala ameneyu. Kaya abwera kaya sabwera koma ndi one tinathana kalekale. He’s just a useless man

Utsiru
5 years ago

Azimayi a dpp, odi ukoooo!! Kpnzekani sambani, Maliseche akubwera muzikavina nawoooo

Fake Trump
Fake Trump
5 years ago

He’s still in US wasting taco money while the country begs for aid from
melania to fix broken schools. You pet are indeed a sit holes country

Tatopa
Tatopa
5 years ago

Thank yoU Melania Trump for cutting Mr and Mrs Maliseche’s trip short, you just saved us a lot of Tax payers money,

happy
happy
5 years ago

Join the discussion…Kkkkkkkkkkkk pitala

#DzukaniAmalawi
#DzukaniAmalawi
5 years ago

Is it just my observation that for the past UNGA no single African head of state has made impact on the stage worth BBC , Al Jazeera or CNN mention. It seems their speeches are so lukewarm and uninspiring that no one takes notice. In fact these African leaders are so ineffective at their own regional body AU that no one in Africa is interested.

Tatopa
Tatopa
5 years ago

It’s just a big boys club, nothing to write home about it’s a serious waste of resources

BigMan
BigMan
5 years ago

No need to return to Malawi Mr President, you being here makes very little impact. Mchacha and his brigade of cadets are running the show with or without you.

gwenenthe mwale
gwenenthe mwale
5 years ago

total shame. the whole educated minister wearing colours of a political party in AMERICA. as if she is in mponela near kasangadzi river. my foot

braveheart
5 years ago

…thus what we call loyalty

Patrick Mbewe
Patrick Mbewe
5 years ago

2017 there was not a single fatal air accident in the whole world. So far 200 plus have died this year. Just statistics sindikunena kuti awanso ndege yao igwe. Koma zitatero mwina Malawi tingapulumuke mu gehena tili lero. May kwatalika amalawi tili pa moto ndalama akuseweretsa akuluwa mapwevupwevu

Chakwera
Chakwera
5 years ago
Reply to  Patrick Mbewe

Inu ndinu achitsiru othelatu,how can a normal person wish his leader death?….muzipita ku Zomba basi

pathfinder
pathfinder
5 years ago
Reply to  Chakwera

Not only his leader but his fellow human being. Amalawi nsanje yanu yafika potero mpaka? Mwagulitsa umunthu wanu chifukwa cha ndale? Ayi ndithu patrick mbewe inensotu mfunda wanga ndi mbewe ndiye ndikukupemphani kuti muchepetse nkwiyo wanu ndithu, ukuwonongetsa chikhalidwe chanu chenicheni cha chimalawi. Ngati wachibale wanu akamwalira kaya pa ngozi kaya pa matenda, inu ndikumava chisoni ndikumalira, ndimomwemonso achibale a Peter Mutharika ndi anthu ena akwere nawo mundegewo azamvere kupweteka ngati iwo atamwalira. Ndikhulupilira thembelero mwaliika pa anthu awa silibwera mubanja lanu first, chifukwa nthawi zambiri ndimmene zimakhalira. Kukumba chidzenje kuti wina agweremo, umagweramo ndi iwe kapena okondedwa wako instead.

Noxy
5 years ago
Reply to  pathfinder

Kusavinidwa

GIRIMOTI
GIRIMOTI
5 years ago
Reply to  Patrick Mbewe

MALISECHE AKUBWERAAAAAA!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!

Lovemore
Lovemore
5 years ago
Reply to  Patrick Mbewe

Amwene umunthu mulibe and you don’t even know how serious is a plane crash ngati kuli kulodzedwa akulodzani kwambiri. Uzaziwona m’mene zimakhalira when you are involved in the situation you are now proud of.
Kumakhala serious aMalawi.

Samuel
Samuel
5 years ago
Reply to  Lovemore

Dzenje walikumbali Patrick Mbewe ulitseka wekha. Pitala ndi anthu onse afika bwino bwino ndipo 2019 awinanso chisankho. Akakukomula mtima Mulungu udzaziona.

Noxy
5 years ago
Reply to  Lovemore

Wishing someone death is a total sign of immaturity

Read previous post:
Cattle rustler jailed 5 years, herd boy gets 4 years imprisonment

A cattle rustler in Chikwawa Mike Sintidu - a well known butcher in the district-  has been handed a five-year- jail sentence ...

Close