Email a copy of 'Mutharika to welcome Uladi and BJ Mpinganjira in DPP' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Mutharika to welcome Uladi and BJ Mpinganjira in DPP' to a friend
The Democratic Progressive Party (DPP) ‘Government’s costly stunts are too much’ is the verdict of the editorial comment in Malawi’s...
Uladi Mussa 50 passports B J Mpinganjira Makolija both of them dead woods. Uladi kaya ukuti wathawira ku Talisi koma msomba ikubweretsa mpakana udzayankha ya ma passport, D P P ikuweta nkhuku zoleka kuikila pomwe M C P ikuweta misoti kuti iyikile koma 2019 kuli ntchito. A Uladi chonde ndalama za Cashgate muwafotokonzere bwino bwino a zanu iwo so akufutokonzerani pakuti mwakumana tsopano. Koma M C P yakutsekulani m’mimba mpakana kukasolola Makolija
Anyamatawa ndi owinawina kale nchifukwa chake MCP mmimba kuti buuuuuuuuuuu. Paja ndale za MCP ndi za retribution and vengeance,. In politics anything can happen. Koma DPP ndikuitaira kamtengo chifukwa imasewera ndale moipa zedi. DPP leads in politics and others follow. Enanu tawirikizani kumenyana ndikutukwanana mchipani mwanumo. Ife a DPP tili pheeeee, tikumwa yoghurt.
Uladi has been an MP ever since he joined real politics. Whichever party he stands for he is always elected to parliament. Even if he stands for MCP this time he will still make it to parliament. This is why MCP feels pain to hear that Uladi is joining the party which MCP hates most.
Malawi has run out of ideas. The politics of Malawi makes one want to vomit. Why bring back politicians that have zero track record. No! guys you can do better than this. Bringing back corruption riddled politicians for what now?
Mmene ndikuonera ineyo ngati mbwiwi pa ndale. Dpp yasowa chochita basi, and dpp tsopano ililbe nzeru nzeru zatha. Anthuwa Profesa Bingu Wamtharika anawachotsa mchipani. Tsono a dpp muziona kuti komwe akuchokera wachikeranji. Mudzi ukamalandila anthu amisala okhaokha mudzio watha basi.
Uladi Mussa, Brown Mpinganjira are rolling stones. These are useless and unprincipled politicians not even worthy second mention. They are here for their personal survival. Uladi has been in parliament since 1994. What impact has he made to Malawians.
DPP, UDF and PP are parties of recycled cashgaters. Malawi will never change. Church needs to rise up and pray for the healing and deliverance of the nation and also deal with the principality ruling that region. The problem is spiritual and if not dealt with from the root, poverty, hardship, wickedness and backwardness will continously prevail.
Madeya as a Chair used to say
Malawi dziko lomvetsa chisoni,,dziko loti silidzatukuka.Brown Mpinganjira what else do you have to offer mother Malawi other than stealing from government coffers.Or do you intend to divorce mai ake a Jill and snatch someone’s wife mukaba ndalama Ku bomako??I hear you are evangelist, why can’t you concentrate on spreading the word of God??Know that you are past your prime,retire hounarably .And to you DJ dzidzidzi(Peter Muthalika) open your eyes,osamangolandila zilizonse mchipani.These two guyz won’t bring any change to your camp.watch out!!!
This is laughable. i can laugh out loud and loud. When shall these wonders end?