Email a copy of 'Nankhumwa back in Ndirande on Sunday to follow up on rally pledges' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

22 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
ndele
ndele
5 years ago

vuto lake ndiloti cipani cili cose cosankhidwa siciimapitiliza citukuko comwe zipani za mbuyomu cinayamba conco zimati zikayambika ,zimalekezera panjila koma izi za cipatala ku mbalanya kwa nfumu nyambi ku mangoci. cipatala coyamba 1997 mpaka lelo sanasekule anthu kulila ndi cisoni coti umoyo wa a anthu sukuyanganilidwa and there come ati minister of health kuti akudikila equipment – timati zipangizo please mukuuza anthu akumidzi osati olankhula cizungu pls atupele, not only that, kuli ma nurse ,ma dokta osalembedwa ncito ,akungokhala and here with your fat ass kumati tiwalemba shit pa dzana pajaunakafola ndi vice wa india next thing he comes here… Read more »

Change is needed
Change is needed
5 years ago

All this is happening because DPP is slowly losing confidence. They are in doubt. Did we realy convinced people to vote for us? Even their president has the same problem. You are doing little.
Panopa magetsi ndi othima. M’makata chithimireni dzulo. Makhwala zipatala mulibe. Madzi chitulukireni kaya liti komanso omatuluka anthu akugona. Even the few supporters remaing in the party are walking with their heads down. Akamatuluka m’nyumba atavala makaka achipani magetsi atathima madzi akukapepha kwa neighbour komwe kuli mpope iwo atalephera kutunga kamba koti madzi amatuluka iwo akugona ndipo asiyanso. Manyazi enieni. Masapota oterewa, olo mutawayendera tsikunditsiku palibe chingasithe.

Malawis future
Malawis future
5 years ago

Lack of strategy my brother Nankhumwa, you are a good guy but not the extent of bn our leader, we need a risk taking kind of a leader who can shake things , who can run government business unusual way. May the best team win in 2019 .

Nzika ya Malawi
Nzika ya Malawi
5 years ago

Yautsiru! Where were you the past 5 years? Those funds are our taxes, wina asamakunamizeni kuti wakuchirani chitukuko zili ndalama zanu zomwe. Vote yanunkhira, ogona adzuka! Agogo ako amanamizanso ma civil servant ku Mzuzu.

Make Malawi Great
Make Malawi Great
5 years ago

Your really taking the people of Ndirande for fools with your frequent rallies? Where have u been all the months? donating bikes in Lomwe belt? Wake up Malawians and chase away these politicians before they disappear after getting your votes. Their neckback is getting fatter with stolen money!!

sato
sato
5 years ago

Mega rally sinaphule kanthu ndi chifukwa chake aNankhumwa akubwereranso Ku Ndirande. Mwabera a Malawi nthawi yonseyi pano ndiye muwafuna. Mukhaula simunati anzanu akudutsa kumalo kamodzi ndi mfundo zomveka. Mumatamba kuyera kuyiwala kuti dzuwa lituluka.

Kalulu Wadwala
Kalulu Wadwala
5 years ago

The problems of people of ndix have been there all along . Why now showing concerns when we have been suffering? We want this to happen when a new govt has been ushered in not during campaign time.

Tiyeni
Tiyeni
5 years ago

Too little too late!

Labwino Lowala
Labwino Lowala
5 years ago

Why haven’t DPP undertaken these projects already over the past 4 years? We are tired of these take promises DPP. Dzimvele Pumbwa Pakila (DPP) has failed Malawians big time. It’s not fair to Malawians for DPP to be eating the meat themselves while putting mere meat oil on people’s mouths. Time is up. You had 4 years to undertake these developments Kondwani what have you done apart from enriching yourselves and growing scombingos? You are lying to Malawians and that’s not good. Change is enivitable Kondwani and your cronies. You are bad people who don’t care about mother Malawi.

Grova
Grova
5 years ago
Reply to  Labwino Lowala

I am sure people of Ndirande will be given a raw deal. Ask area 24 people in Lilongwe. The road that was constructed some 6 months ago is already in shambles. Anangopaka paka matope ndi mchenga, where was the road authority in regard, where were the city engineers ? . Chinyenga mpnunzitsi basi. Is this what Malawians want? Please lets love our country regardless of where we are coming from. Ndine Mlomwe yes and I love my country and would want to see it develop in every region. Ife amene tayendafe timachita manyazi ndi zochitika kwathuko

Salah
5 years ago

Anthu a Ku ndikisi mwatani? Tawonani George Malemia akubwelaso kodi inu simamuvesa inu? Chabwino ndikisi azayivesa bwino pa 21 may 2019

Read previous post:
Malawi NGO Bill raises concern: Endangers the existence of civil society

Civil Society Organisations (CSOs) have condemned government’s attempts to close down human rights NGOs through its draconian proposed Bill. The...

Close