Email a copy of 'Nepman does not claim owning hit song ‘Chilawe Changachi’ – Manager' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Nepman does not claim owning hit song ‘Chilawe Changachi’ – Manager' to a friend
Just when you thought you had worn out the repeat button with “Msati Mseke”, Blantyre gospel musician Patience Namadingo is...
Oh shame Black Nina!!!!
Nepman n munthu wankulu
Ufuna achite kukutenga Ku show kuti nawenso utchuke? Unatchuka kale poyimba ndi otchuka kale nepman and’nso ukuwonjezera kutchukako pamene ukulimbana nayepa. Ine kuyamba kudziwa kuti kuli oyimba dzinalake lakolo.
Musiye mwana wa mugetto. oziwa kupeka yekha
Chilawe! Chilawe changachi! Tachilawe chikondi changachi! Chokoma ngati chakumangochi!
Black Nina kkkkkkk chilawe changa!!!!!!! Ukayenda ndi mwana wayenda wekha!!!!! Nep Man ndidamuziwa kalekale Akumaimba kwa Kampa ku ntonjani! Watchuka kamba kakulimbikila kwake!!!!! Kp it up Nep Man,,,,,,,,,,
Nina ngati umatha kuyimba tulutsa yako album. Nepman ndi dolo I we ndi kape. Nyimbo ukunenayo timaveraso pa chorus basi zako za unigers zopanda pake. Wayamba liti kuyimba?
Black Nina, Collabo ndi Collabo imakhala yopanda mwini….ndipo if you search it using your name as a prefix kkkk Google won’t bring the song up, unless we use nepman as a prefix
Black Nina , how many songs do u hv? Osangotulutsa album bwanji tigule ngati tikufuna
Oimba achiYo.. paMalawi. Nepman please beef him amve kuwawa