Email a copy of 'Nkhotakota people demand transfer of DC : Malawi govt given 10 days ultimatum' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

41 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
Vitu
Vitu
8 years ago

Felix Mkandawire is mbuzi ya DC. The problem with local government is that they know vuto lamunthu but continue kumudalira. Felix tidamuthamangitsa kuno ku Dowa we had to close his office. Munthuyu ndi mulesi komanso mbava yothelatu uphatikiza mowa too much . He is not a DC material akuchititsani manyazi a nduna. Anduna athandizeni anthu a KK ali mmavuto.

Mhango
8 years ago

Mtumbuka apa wapezeka.mtundu okonda kusolola ndi kachasu.leave kk alone pitani mukagulitse malo akukaya ku north not kk land. Anthu a kk samapita ku euthini or enukweni kukagalittsa malo.adhere to ten day ultimatum or else mukakoke mu office or kunyumba kwawo.the honey moon is over!! Pliz kk pple wake up enough iz enough

Private detective
Private detective
8 years ago

We will not have mercy on or its not a matter of puting your phone numbers or chamba or tribelism or how educated you are what ever you have been doing God almighty will reveal your foolishnes selfishnes this is just the begining or you want us to send the shooting of videos of what you have doin to the mbc if you challenge tell us? Idiots always dont accept idiotism we not fools we have to start afresh enough is enough

Nyambosi
8 years ago

Ndingakumanyani Chala Anthu Aku KK kuti ndinu wakuona.ndingagulitsa malo mwachiphuphu pakuti ndimatumidwa ndimabwana amene ali mupetition.walawala ndi gowokeleni ine ndekha.apa ndawona kuti atumbuka tili selfish nanga ofesi ya DC YONSE tokha mpakana cleaner, messenger

Moi
Moi
8 years ago

The truth behind the matter is that Akotakota ali ndi vuto LA Obwera syndrome, the story behind the matter is that mayina anatuluka mix, and some notable (that’s what they think they R) Kotakotas mayina awo sanapezeke and they started having meetings against obwera omwe malo apasidwa! and these pipo akunamizira transparency! Mind you ngati kuli malo osatukuka NDE ndikumeneko and its due to this obwera syndrome!! The MP Mazizi, is the best don’t insult him!! he is not behind this!! walandira petition on behalf of the Ministry that’s all.. the place needs developments osati tizisakasa pa boma panji pomati… Read more »

Manuel chavinda
8 years ago

Talakwira ife anthu a kk powapondeleza kwabasi.ife atumbuka timaona kuti ndife mashasha koma ayi ndife mazoba.kk yalankhula apa ndiye anduna tithazeni kutisamusa mofulumira zinthu zisanafike povuta

Nedson Trouble Jere
8 years ago

kwakwangwa and mache you are heroes.These people dd not employ themselves.The problem is that kk pple chamba too and the sad part of it is that an mp joins chamba smokers.I have huge respect for MCP MPs but this peter mazizi the mental faculty is not alright.The problem is with the chewas if you tell them to go for break at school they go home for good.Ngati mwapsa mtima ipsani mtima zenizeni and call 0 888 185 448.

bj
bj
8 years ago

fools of people, instead of dreaming how to acquire wealthy and manage the limited resources we have, you are busy tussling. Many people are jobless in your district and you take it as a very normal situation- fools. Fighting for positions won’t help you either, somebody was denied of land allocation, hence, mobilizing innocent en un educated people to rally for such demonstrations. I don’t think such area will suffice everybody in Nkhotakota district. Maybe it might be the member of parliament who is behind this- foolish ego…

Gabriel
8 years ago

DC Mkandawire anatenga One Mita Kupita Nayo Ku RSA

maximo
maximo
8 years ago

Tabwelelanso ku mzimba tizizamwa chill pa sankhawekha ndi pa kettie mkunkha,tizikacheka patabwa ku nkhalango basi we the ngoni we miss you,asiye osuta chamba kumeneko

Read previous post:
Malawians heading back to South Africa were being trafficked

The bus, police intercepted in Lilongwe two days ago full of passengers, with some standing, on its way to South...

Close