Email a copy of 'Nomads snub Sidik Mia cash donation over politicking' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

11 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
B Mnthali
B Mnthali
6 years ago

I think FIFA rules do not allow politicians to have influence in football matters through such donations as this would compromise the position of Wanderers. Assuming another rich DPP politician offered a higher donation than MIA on condition that they do not take MIAs money, what would happen? It would be a tag of war with Wanderers being torn apart.

Only heads of state, in their capacity can sponsor teams as they are national fathe/mother figures.

Nyerere 2
Nyerere 2
6 years ago

Mbuzi za anthu manoma ma politician ali thoo mu team sichifukwa ma sponsor akutayilani game. James chuma,gaffar ndi alimi?

Keen Observer
Keen Observer
6 years ago

Cheap politics Mr Mia anali kuti all this time? Komanso nawo a Wanderers osangoti ngati ndalamazo bwanji?

Masuzgyo
Masuzgyo
6 years ago

There is a strong group of Moslems who are against MIA pairing with CHAKWERA and later alone SUPPORTING MCP and that is why sakugona tulo trying to reach out even to footballers and vendors.
KOMATU ziliko ziliko isiyeni mijomba atana naye mkaladiyu.

Noria
6 years ago
Reply to  Masuzgyo

Osakapatsa a mwenye anzako akugona mmizikitiwa! Foolish Indian.

Maunits
Maunits
6 years ago

Zabodza zimenzo Donation ndi donation ngati Noma inafuna kupanga withdrawal a Gaffar analikuti mantha ndi Mia DPP Munya muona.

Hatton
Hatton
6 years ago

Bola a Miawa asakweze mtengo wa mang’ina ndi utsilu omwe akupanga ndi ndalama akutolera mwa amwenye mu Limbe mu.

Youna
Youna
6 years ago

Azibweretse kuno ife tizilandira. Afterall ndalama siikhala ndi dzina la munthu.

Amboziye
Amboziye
6 years ago

Its you politicians amene mmaononga ma team athuwa so you want to destroy Nomads just like Muluzi destroyed Bullets, take your money to MCP akalipile ma bill amadzi komanso Lilongwe city council outstanding city rates

Lupwito
Lupwito
6 years ago
Reply to  Amboziye

In Agreeing with you Ambozi, mapaxi ake shehe ameneyu, aileke NOMA ndipo olo nkanakhala ineyo sindikanalola kupusa kwakeko… akapereke khobili lakelo ku ESCOM/EGENCO ndi kwinako osati asimbwe ndikukulapo ntima pachi team chathuchi shupit………Bloody Money!

Chikulamayembe
6 years ago

Azikhuta amenewo

Read previous post:
Malawi govt set up unit to confiscate all ‘Cashgate assets’, recover money

Malawi government has launched  a special unit that will be responsible for confiscating wealth proven to have originated from proceeds...

Close