Email a copy of 'Nomads surrender title at Chitowe as Nyasa Bullets are Malawi football kings' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Nomads surrender title at Chitowe as Nyasa Bullets are Malawi football kings' to a friend
Malawi Under-20 national football team which to Lusaka, Zambia to participate at the 2018 Under-20 Cosafa Championship without training camp...
This reporter is a Nyerere fan, weniweni wa Manoma ndithu, too biase popanga report
Ma ref anali atakonzedwa kale ndi Bullets!
This reporter is absolutely biased, but i am not surprised though. Jeromy Kadewere ndi wa noma. Simudzampeza atalemba nkhani yabwino ya Bullets olo itachita bwino. Onani apa the same yesterday Bullets yawina koma sakulembapo kanthu. Kodi manomawo mukufuna apatsidwe ma penalty angati mu season imodzi? Lowelika lomweli chigoli chawo chowinila chinali cha penalty, mukufuna kundiuiza kuti mpaka pano simukudziwa kuti osewera a noma amakonda kuzigwetsa mu eighteen yard box, makamaka akamaona kuti zinthu zikuwabvuta?
kkkkkkkkkk mwagwa nayo kodi inuyo nokha basi muzilandira ma penalty shame on you count how many penalties have you been given this season alone, and to you stupid reporter your reporting shows a very biased reporter you are
LOOKING AT THE FACES OF OUR PLAYERS ABOVE (PHOTO );THEY LOOK VERY VERY ANGRY —WERE THEY FORCED TO PLAY FOOTBALL ?? TELL THEM EVERYTHING YOU DO WITH ANGER: BITTERNESS ; FRUSTRATION
IS NO GOOD –RATHER DO EVERYTHING WITH A SMILE ON YOUR FACE ‘—MAKES THE CREATOR HAPPY !! GOALS SHOWER !!